Salimo 24
Salimo la Davide.
1Dziko lapansi ndi la Yehova ndi zonse zimene zili mʼmenemo,
dziko ndi onse amene amakhala mʼmenemo;
2pakuti Iye ndiye anayika maziko ake pa nyanja
ndi kulikhazika pamwamba pa madzi.
3Ndani angakwere phiri la Yehova?
Ndani angathe kuyima pa malo ake opatulika?
4Iye amene ali ndi mʼmanja moyera ndi mtima woyera,
amene sapereka moyo wake kwa fano
kapena kulumbira mwachinyengo.
5Iyeyo adzalandira madalitso kwa Yehova
ndipo Mulungu mpulumutsi wake adzagamula kuti alibe mlandu.
6Umenewo ndiwo mʼbado wa amene amafunafuna Yehova;
amene amafunafuna nkhope yanu, Inu Mulungu wa Yakobo.
Sela
7Tukulani mitu yanu inu zipata;
tsekukani, inu zitseko zakalekalenu,
kuti Mfumu yaulemerero ilowe.
8Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?
Yehova Wamphamvuzonse,
Yehova ndiye wamphamvu pa nkhondo.
9Tukulani mitu yanu, inu zipata;
tsekukani, inu zitseko zakalekalenu,
kuti Mfumu yaulemerero ilowe.
10Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?
Yehova Wamphamvuzonse,
Iye ndiye Mfumu yaulemerero.
Sela
Den almægtige Konge
1En sang af David.
Jorden og alt, hvad der er på den, tilhører Herren,
hele verden og alle, som bor i den.
2Han grundlagde jorden på verdenshavene,
dens fundament lagde han på havets dyb.
3Hvem kan stige op på Herrens bjerg?
Hvem har lov at gå ind i hans helligdom?
4De, som har rene motiver og gør det gode,
som ikke tilbeder afguder eller sværger falsk.
5Sådanne mennesker bliver velsignet af Gud
og nyder godt af hans trofasthed og godhed.
6Kun de må komme ind i Herrens nærhed
og tilbede Jakobs Gud.
7Luk de ældgamle døre vidt op,
gør plads i byens indgangsport,
så den almægtige Konge kan komme ind.
8Hvem er den almægtige Konge?
Det er Herren, som er stærk og mægtig.
Det er Herren, som vinder enhver kamp.
9Luk de ældgamle døre vidt op,
gør plads i byens indgangsport,
så den almægtige Konge kan komme ind.
10Hvem er den almægtige Konge?
Det er Herren, som styrer alt.
Han er den almægtige Konge.