Salimo 23
Salimo la Davide.
1Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
2Amandigoneka pa msipu wobiriwira,
amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
3amatsitsimutsa moyo wanga.
Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo
chifukwa cha dzina lake.
4Ngakhale ndiyende
mʼchigwa cha mdima wakuda bii,
sindidzaopa choyipa,
pakuti Inu muli ndi ine;
chibonga chanu ndi ndodo yanu
zimanditonthoza.
5Mumandikonzera chakudya
adani anga akuona.
Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta;
chikho changa chimasefukira.
6Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata
masiku onse a moyo wanga,
ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova
kwamuyaya.
우리의 목자가 되시는 여호와
(다윗의 시)
1여호와는 나의 목자시니
내가 부족함이 없으리라.
2그가 나를 푸른 풀밭에 쉬게 하시고
잔잔한 물가로 인도하시며
3내 영혼을 소생시키시고
자기 이름을 위하여
나를 의로운 길로
인도하시는구나.
4내가 죽음의
음산한 계곡을 걸어가도
두려워하지 않을 것은
주께서 나와 함께하심이라.
주의 지팡이와
막대기가 나를 지키시니
내가 안심하리라.
5주께서 내 원수들이 보는 가운데
나를 위해 잔치를 베푸시고
23:5 또는 ‘기름으로 내 머리에 바르셨으니’나를 귀한 손님으로
맞아 주셨으니
내 잔이 넘치는구나.
6주의 선하심과 한결같은 사랑이
평생에 나를 따를 것이니
내가 여호와의 집에서
영원히 살리라.