Masalimo 136 – CCL & OL

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 136:1-26

Salimo 136

1Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.

Pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

2Yamikani Mulungu wa milungu.

Pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

3Yamikani Ambuye wa ambuye,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

4Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

5Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

6Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

7Amene anapanga miyuni ikuluikulu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

8Dzuwa lilamulire usana,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

9Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

10Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

11Natulutsa Israeli pakati pawo,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

12Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

13Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

14Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

15Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

16Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

17Amene anakantha mafumu akuluakulu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

18Napha mafumu amphamvu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

19Siloni mfumu ya Aamori,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

20Ogi mfumu ya Basani,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

21Napereka dziko lawo ngati cholowa,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

22Cholowa cha mtumiki wake Israeli;

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

23Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

24Amene anatimasula kwa adani athu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

25Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

26Yamikani Mulungu wakumwamba,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

O Livro

Salmos 136:1-26

Salmo 136

1Deem graças ao Senhor porque ele é bom,

porque o seu amor é eterno.

2Deem graças a Deus que está acima de todos os deuses;

porque o seu amor é eterno.

3Louvem aquele que é o Senhor dos senhores;

porque o seu amor é eterno.

4O único que faz milagres poderosos;

porque o seu amor é eterno.

5Fez o universo pela sua sabedoria;

porque o seu amor é eterno.

6Foi ele quem distribuiu os mares sobre a superfície da Terra;

porque o seu amor é eterno.

7Criou os grandes astros;

porque o seu amor é eterno.

8Fez o Sol para dar luz e marcar o tempo durante o dia;

porque o seu amor é eterno.

9Fez a Lua e as estrelas para governarem a noite;

porque o seu amor é eterno.

10Ele tirou a vida aos filhos mais velhos das famílias do Egito;

porque o seu amor é eterno.

11Retirou o seu povo Israel do meio daqueles que os escravizavam;

porque o seu amor é eterno.

12Fê-lo com todo o seu poder e autoridade;

porque o seu amor é eterno.

13Fez com que o mar Vermelho se abrisse em dois;

porque o seu amor é eterno.

14Levou Israel a atravessá-lo em seco;

porque o seu amor é eterno.

15Deixou que o exército do Faraó se afogasse nesse mesmo mar;

porque o seu amor é eterno.

16Depois guiou o seu povo através do deserto;

porque o seu amor é eterno.

17Derrotou grandes e poderosos reis;

porque o seu amor é eterno.

18Tirou a vida a reis famosos;

porque o seu amor é eterno.

19A Siom, rei dos amorreus;

porque o seu amor é eterno.

20E a Ogue, rei da Basã;

porque o seu amor é eterno.

21A sua terra foi dada como propriedade aos israelitas;

porque o seu amor é eterno.

22Foi-lhes dada como herança, pois é um povo que serve o Senhor;

porque o seu amor é eterno.

23Deus lembrou-se da nossa grande fraqueza;

porque o seu amor é eterno.

24Salvou-nos dos nossos inimigos;

porque o seu amor é eterno.

25Ele sustenta todos os seres vivos;

porque o seu amor é eterno.

26Louvem o Deus dos céus;

porque o seu amor é eterno.