Salimo 131
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide.
1Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza,
maso anga siwonyada;
sinditengeteka mtima
ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
2Koma moyo wanga ndawutontholetsa
ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa,
moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
3Yembekeza Yehova, iwe Israeli,
kuyambira tsopano mpaka muyaya.
Salmo 131
Cántico de los peregrinos. De David.
1Señor, mi corazón no es orgulloso,
ni son altivos mis ojos;
no busco grandezas desmedidas,
ni proezas que excedan a mis fuerzas.
2Todo lo contrario:
he calmado y aquietado mis ansias.
Soy como un niño recién amamantado en el regazo de su madre.
¡Mi alma es como un niño recién amamantado!
3Israel, pon tu esperanza en el Señor
desde ahora y para siempre.