Masalimo 131 – CCL & BPH

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 131:1-3

Salimo 131

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide.

1Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza,

maso anga siwonyada;

sinditengeteka mtima

ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.

2Koma moyo wanga ndawutontholetsa

ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa,

moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.

3Yembekeza Yehova, iwe Israeli,

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

Bibelen på hverdagsdansk

Salmernes Bog 131:1-3

Hvilen i Gud

1En valfartssang af David.

Herre, mit hjerte er ikke hovmodigt,

jeg knejser ikke med nakken,

jeg siger ikke mere, end jeg kan stå inde for,

jeg har ikke urealistiske forestillinger,

2men jeg har fundet hvile og ro i dig.

Som et lille barn er trygt hos sin mor,

har min sjæl fundet hvile hos dig.

3Israel, sæt trygt jeres lid til Herren,

stol på ham evigt og altid.