Masalimo 13 – CCL & NRT

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 13:1-6

Salimo 13

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

1Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?

Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?

2Ndidzalimbana ndi maganizo anga

ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti?

Mpaka liti adani anga adzandipambana?

3Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.

Walitsani maso anga kuti ndingafe;

4mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”

ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.

5Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;

mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.

6Ine ndidzayimbira Yehova

pakuti wandichitira zokoma.

New Russian Translation

Псалтирь 13:1-7

Псалом 13

(Пс. 52)

1Дирижеру хора. Псалом Давида.

Сказал безумец в сердце своем:

«Нет Бога».

Они развратились, гнусны их дела;

нет делающего добро.

2Господь взирает с небес на людей,

чтобы увидеть, есть ли понимающий,

ищущий Бога.

3Все сбились с пути,

все, как один, развратились;

нет делающего добро,

нет ни одного.

4Неужели не вразумятся делающие зло –

те, кто поедает мой народ, как хлеб,

и Господа не призывает?

5Там их охватит страх,

потому что Бог на стороне праведных.

6Вы осмеяли надежды нищих,

но прибежище их – Господь.

7О, кто дал бы с Сиона спасение Израилю!

Когда Господь восстановит Свой народ,

пусть ликует Иаков и радуется Израиль!