Masalimo 13 – CCL & KLB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 13:1-6

Salimo 13

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

1Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?

Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?

2Ndidzalimbana ndi maganizo anga

ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti?

Mpaka liti adani anga adzandipambana?

3Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.

Walitsani maso anga kuti ndingafe;

4mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”

ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.

5Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;

mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.

6Ine ndidzayimbira Yehova

pakuti wandichitira zokoma.

Korean Living Bible

시편 13:1-6

속히 도와 달라는 기도

(다윗의 시. 성가대 지휘자를 따라 부른 노래)

1여호와여, 언제까지

나를 잊으시겠습니까?

영원히 잊으실 작정이십니까?

나에게 주의 얼굴을

언제까지 숨기시겠습니까?

2내가 언제까지 번민하며

하루 종일 슬퍼해야 합니까?

언제까지 내 원수들이

나를 이기겠습니까?

3여호와 나의 하나님이시여,

나를 바라보시고 응답하소서.

내가 죽음의 잠을 자지 않도록

내 눈을 밝혀 주소서.

4내 원수들이

“우리가 너를 이겼다”

하고 말하지 못하게 하소서.

그들이 내가 넘어진 것을

기뻐하지 못하게 하소서.

5내가 한결같은

주의 사랑을 의지하고

주의 구원을 기뻐하겠습니다.

6여호와께서 나를

후하게 축복하셨으니

내가 그를 찬양하리라.