Masalimo 128 – CCL & NRT

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 128:1-6

Salimo 128

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Odala ndi onse amene amaopa Yehova,

amene amayenda mʼnjira zake.

2Udzadya chipatso cha ntchito yako;

madalitso ndi chuma zidzakhala zako.

3Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka

mʼkati mwa nyumba yako;

ana ako adzakhala ngati mphukira za mitengo ya olivi

kuzungulira tebulo lako.

4Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa

amene amaopa Yehova.

5Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni

masiku onse a moyo wako;

uwone zokoma za Yerusalemu,

6ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako.

Mtendere ukhale ndi Israeli.

New Russian Translation

Псалтирь 128:1-8

Псалом 128

1Песнь восхождения.

Много раз притесняли128:1 Или: «причиняли страдания». Также в ст. 2. меня с юности, –

пусть скажет Израиль, –

2много раз притесняли меня с юности,

но не одолели.

3На спине моей пахали пахари,

проводили свои длинные борозды.

4Господь праведен:

Он разрубил узы нечестивых.

5Пусть постыдятся и повернут назад

все ненавидящие Сион.

6Пусть будут они как трава на крыше дома,

которая высыхает прежде чем будет вырвана.

7Жнец не наполнит ею руки своей,

и вяжущий снопы не соберет ее в пригоршни.

8Проходящие мимо не скажут:

«Благословение Господне на вас!

Благословляем вас именем Господним».