Salimo 128
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1Odala ndi onse amene amaopa Yehova,
amene amayenda mʼnjira zake.
2Udzadya chipatso cha ntchito yako;
madalitso ndi chuma zidzakhala zako.
3Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka
mʼkati mwa nyumba yako;
ana ako adzakhala ngati mphukira za mitengo ya olivi
kuzungulira tebulo lako.
4Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa
amene amaopa Yehova.
5Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni
masiku onse a moyo wako;
uwone zokoma za Yerusalemu,
6ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako.
Mtendere ukhale ndi Israeli.
Псалом 128
1Песнь восхождения.
Много раз притесняли128:1 Или: «причиняли страдания». Также в ст. 2. меня с юности, –
пусть скажет Израиль, –
2много раз притесняли меня с юности,
но не одолели.
3На спине моей пахали пахари,
проводили свои длинные борозды.
4Господь праведен:
Он разрубил узы нечестивых.
5Пусть постыдятся и повернут назад
все ненавидящие Сион.
6Пусть будут они как трава на крыше дома,
которая высыхает прежде чем будет вырвана.
7Жнец не наполнит ею руки своей,
и вяжущий снопы не соберет ее в пригоршни.
8Проходящие мимо не скажут:
«Благословение Господне на вас!
Благословляем вас именем Господним».