Masalimo 126 – CCL & NRT

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 126:1-6

Salimo 126

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni,

tinali ngati amene akulota.

2Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka;

malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe.

Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti,

“Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”

3Yehova watichitira zinthu zazikulu,

ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.

4Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova,

monga mitsinje ya ku Negevi.

5Iwo amene amafesa akulira,

adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.

6Iye amene amayendayenda nalira,

atanyamula mbewu yokafesa,

adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe,

atanyamula mitolo yake.

New Russian Translation

Псалтирь 126:1-5

Псалом 126

1Песнь восхождения Соломона.

Если не Господь строит дом,

то напрасно трудятся его строители.

Если не Господь охраняет город,

то напрасно бодрствует страж.

2Напрасно вы встаете рано

и сидите допоздна,

тяжелым трудом добывая себе еду,

потому что возлюбленному Своему посылает Он сон126:2 Или: «ведь тем, кого любит, Он дает все необходимое даже во сне»..

3Дети – наследие от Господа,

и плод чрева – Его награда.

4Что стрелы в руке воина,

то сыновья, родившиеся у молодых.

5Блажен человек,

чей колчан наполнен ими.

Не постыдятся они,

когда будут говорить с неприятелями

в воротах города126:5 Ворота города были центром всей общественной жизни, в них проходили и судебные разбирательства..