Masalimo 126 – CCL & BDS

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 126:1-6

Salimo 126

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni,

tinali ngati amene akulota.

2Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka;

malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe.

Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti,

“Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”

3Yehova watichitira zinthu zazikulu,

ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.

4Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova,

monga mitsinje ya ku Negevi.

5Iwo amene amafesa akulira,

adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.

6Iye amene amayendayenda nalira,

atanyamula mbewu yokafesa,

adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe,

atanyamula mitolo yake.

La Bible du Semeur

Psaumes 126:1-6

Semailles et moisson

1Cantique pour la route vers la demeure de l’Eternel126.1 Voir note 120.1..

Quand l’Eternel a ramené ╵les captifs de Sion126.1 Autre traduction : a changé le sort de Sion.,

nous étions comme dans un rêve.

2Alors nous ne cessions de rire

et de pousser des cris de joie.

Alors on disait chez les autres peuples :

« Oh, l’Eternel a fait pour eux ╵de grandes choses ! »

3Oui, l’Eternel a fait pour nous

de grandes choses :

nous sommes dans la joie.

4Viens changer notre sort126.4 Autre traduction : ramène nos captifs., ╵ô Eternel,

comme quand l’eau coule à nouveau ╵dans les lits des rivières du Néguev.

5Qui sème dans les larmes

moissonnera avec des cris de joie !

6Qui s’en va en pleurant ╵alors qu’il porte sa semence

reviendra en poussant des cris de joie, ╵alors qu’il portera ses gerbes.