Salimo 125
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,
limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,
momwemonso Yehova azungulira anthu ake
kuyambira tsopano mpaka muyaya.
3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala
pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama,
kuti anthu olungamawo
angachite nawonso zoyipa.
4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,
amene ndi olungama mtima
5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,
Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa.
Mtendere ukhale pa Israeli.
สดุดี 125
(บทเพลงใช้แห่ขึ้นไปยังเยรูซาเล็ม)
1บรรดาผู้ที่วางใจในองค์พระผู้เป็นเจ้าก็เป็นเช่นภูเขาศิโยน
ซึ่งไม่หวั่นไหว แต่ตั้งมั่นตลอดกาล
2ดั่งภูเขาทั้งหลายรายล้อมเยรูซาเล็ม
องค์พระผู้เป็นเจ้าก็ทรงโอบล้อมประชากรของพระองค์
ทั้งบัดนี้และสืบไปนิรันดร์
3คทาของคนชั่วจะไม่คงอยู่
เหนือแผ่นดินซึ่งเป็นส่วนของคนชอบธรรม
มิฉะนั้นคนชอบธรรม
จะลงมือทำผิด
4ข้าแต่องค์พระผู้เป็นเจ้า ขอทรงดีต่อผู้ที่ทำดี
ต่อผู้ที่มีจิตใจเที่ยงธรรม
5แต่ผู้ที่หันไปสู่ทางคดเคี้ยว
องค์พระผู้เป็นเจ้าจะทรงเนรเทศเขาไปพร้อมกับคนทำชั่ว
สันติสุขจงมีแก่อิสราเอล