Salimo 125
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,
limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,
momwemonso Yehova azungulira anthu ake
kuyambira tsopano mpaka muyaya.
3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala
pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama,
kuti anthu olungamawo
angachite nawonso zoyipa.
4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,
amene ndi olungama mtima
5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,
Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa.
Mtendere ukhale pa Israeli.
Псалам 125
Песма поклоничка.
1Они што се у Господа уздају,
јесу као гора Сион – постојана,
довека се помакнути не да!
2Попут гора што Јерусалим окружују,
тако је и Господ око свог народа,
све од сада па за вечност целу.
3Уистину, неће жезло злочинаца владати
над земљом што припада праведнима;
да праведни руке своје не би
неправди пружали.
4О, Господе, добро чини добрима
и онима честитога срца!
5А оне што на своје криве стазе скрећу,
Господ ће одагнати са злотворима.
Мир Израиљу!