Masalimo 125 – CCL & BDS

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 125:1-5

Salimo 125

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,

limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.

2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,

momwemonso Yehova azungulira anthu ake

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala

pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama,

kuti anthu olungamawo

angachite nawonso zoyipa.

4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,

amene ndi olungama mtima

5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,

Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa.

Mtendere ukhale pa Israeli.

La Bible du Semeur

Psaumes 125:1-5

Sécurité inébranlable

1Cantique pour la route vers la demeure de l’Eternel125.1 Voir note 120.1..

Ceux qui ont placé leur confiance ╵en l’Eternel

sont comme le mont de Sion : ╵il n’est pas ébranlé

et subsiste à jamais.

2Comme Jérusalem ╵est entourée par des montagnes,

l’Eternel entoure son peuple

dès maintenant ╵et à jamais.

3Un pouvoir criminel ╵ne pourra dominer

sur le territoire échu en partage aux justes,

afin que les justes n’en viennent pas ╵à prêter eux aussi la main ╵à des actes coupables.

4Fais du bien, Eternel, ╵à celui qui est bon,

à celui qui a le cœur droit !

5Mais ceux qui se détournent ╵vers des voies tortueuses,

que l’Eternel les chasse

avec tous ceux qui font le mal !

Que la paix soit sur Israël !