Masalimo 121 – CCL & HOF

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 121:1-8

Salimo 121

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Ndikweza maso anga ku mapiri;

kodi thandizo langa limachokera kuti?

2Thandizo langa limachokera kwa Yehova,

wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.

3Sadzalola kuti phazi lako literereke;

Iye amene amakusunga sadzawodzera.

4Taonani, Iye amene amasunga Israeli

sadzawodzera kapena kugona.

5Yehova ndiye amene amakusunga;

Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.

6Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,

kapena mwezi nthawi ya usiku.

7Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;

adzasunga moyo wako.

8Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

Hoffnung für Alle

Psalm 121:1-8

Unterwegs unter Gottes Schutz

1Ein Lied für Festbesucher, die nach Jerusalem hinaufziehen.

Ich schaue hinauf zu den Bergen –

woher kann ich Hilfe erwarten?

2Meine Hilfe kommt vom Herrn,

der Himmel und Erde gemacht hat!

3Der Herr wird nicht zulassen, dass du fällst;

er, dein Beschützer, schläft nicht.

4Ja, der Beschützer Israels

schläft und schlummert nicht.

5Der Herr gibt auf dich acht; er steht dir zur Seite

und bietet dir Schutz vor drohenden Gefahren121,5 Wörtlich: der Herr ist dein Schatten über deiner rechten Hand..

6Tagsüber wird dich die Sonnenglut nicht verbrennen,

und in der Nacht wird der Mond dir nicht schaden.

7Der Herr schützt dich vor allem Unheil,

er bewahrt dein Leben.

8Er gibt auf dich acht, wenn du aus dem Haus gehst

und wenn du wieder heimkehrst.

Jetzt und für immer steht er dir bei!