Masalimo 12 – CCL & HOF

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 12:1-8

Salimo 12

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide.

1Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika;

okhulupirika akusowa pakati pa anthu.

2Aliyense amanamiza mʼbale wake;

ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.

3Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo

ndi pakamwa paliponse podzikuza.

4Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu;

pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”

5“Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu

ndi kubuwula kwa anthu osowa,

Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova,

“Ndidzawateteza kwa owazunza.”

6Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro

monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi,

oyengedwa kasanu nʼkawiri.

7Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo

mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.

8Oyipa amangoyendayenda ponseponse

anthu akamayamikira zochita zawo.

Hoffnung für Alle

Psalm 12:1-9

Gott hält, was er verspricht

1Ein Lied von David, mit einem tief gestimmten Saiteninstrument zu begleiten.

2Herr, komm mir doch zu Hilfe!

Ich kenne keinen Menschen, der dir noch die Treue hält.

Auf keinen kann man sich mehr verlassen.

3Jeder belügt jeden.

Wie leicht kommen ihnen Komplimente über die Lippen,

aber das ist nichts als Heuchelei.

4Herr, rotte diese Schmeichler aus,

ja, bring diese Angeber zum Schweigen!

5Sie prahlen: »Wir erreichen alles, denn wir sind gewaltige Redner;

gegen uns kommt keiner an!«

6»Doch – ich!«, spricht der Herr,

»jetzt will ich eingreifen, denn die Schwachen werden misshandelt,

und die Armen seufzen, weil man ihnen hart zusetzt.

Ich werde die Unterdrückten befreien!12,6 Oder: Ich werde ihnen die Hilfe schaffen, nach der sie sich sehnen.«

7An den Worten des Herrn gibt es nichts zu rütteln.

Sie sind eindeutig und klar, wie durch und durch gereinigtes Silber.12,7 Wörtlich: wie reines Silber, im Tiegel siebenmal geläutert.

8Du, Herr, gibst uns Sicherheit12,8 Oder: Du, Herr, wirst deine Zusagen erfüllen.

und wirst uns für immer vor diesen

selbstherrlichen Menschen beschützen.

9Denn diese Gottlosen machen sich überall breit,

und die Gemeinheit unter den Menschen nimmt ständig zu.