Salimo 12
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide.
1Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika;
okhulupirika akusowa pakati pa anthu.
2Aliyense amanamiza mʼbale wake;
ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.
3Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo
ndi pakamwa paliponse podzikuza.
4Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu;
pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”
5“Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu
ndi kubuwula kwa anthu osowa,
Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova,
“Ndidzawateteza kwa owazunza.”
6Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro
monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi,
oyengedwa kasanu nʼkawiri.
7Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo
mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.
8Oyipa amangoyendayenda ponseponse
anthu akamayamikira zochita zawo.
Dieu tient ses promesses
1Au chef de chœur, un psaume de David, à chanter avec accompagnement de la harpe à huit cordes12.1 Voir note 6.1..
2Au secours, ô Eternel ! ╵Il n’y a plus d’homme pieux,
on ne peut plus se fier ╵à personne.
3Chacun trompe son prochain,
lui disant des flatteries,
la duplicité au cœur.
4Que l’Eternel extermine ╵ces gens aux lèvres flatteuses
et à la langue arrogante.
5Qu’il retranche ceux qui disent : ╵« Notre langue nous rend forts,
nos alliées, ce sont nos lèvres,
qui dominerait sur nous ? »
6Mais l’Eternel dit : ╵« A cause des pauvres ╵qui sont opprimés ╵et des démunis ╵qui vont gémissant,
maintenant, moi j’interviens
pour accorder le salut ╵à ceux qui sont méprisés. »
7Les paroles du Seigneur, ╵ce sont des paroles pures,
c’est de l’argent affiné,
sept fois purifié ╵par le feu dans un creuset12.7 La traduction est incertaine..
8Eternel, toi, tu nous gardes12.8 D’après quelques manuscrits hébreux et l’ancienne version grecque. Texte hébreu traditionnel : tu les gardes.
et tu nous protégeras ╵toujours contre ces individus.
9Tout autour, des méchants rôdent,
la bassesse prédomine ╵parmi les humains.