There is no audio yet for this translation.
Salimo 117
1Tamandani Yehova, inu anthu a mitundu yonse;
mulemekezeni Iye, inu mitundu ya anthu.
2Pakuti chikondi chake pa ife ndi chachikulu,
ndipo kukhulupirika kwa Yehova nʼkosatha.
Tamandani Yehova.
Loading…
Zabbuli 117
1117:1 Bar 15:11*Mutendereze Mukama, mmwe ensi zonna;
mumugulumize, mmwe amawanga gonna.
2117:2 Zab 100:5Kubanga okwagala kwe okutaggwaawo kungi gye tuli;
n’obwesigwa bwa Mukama bwa lubeerera.
Mutendereze Mukama.