Masalimo 117 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 117:1-2

Salimo 117

1Tamandani Yehova, inu anthu a mitundu yonse;

mulemekezeni Iye, inu mitundu ya anthu.

2Pakuti chikondi chake pa ife ndi chachikulu,

ndipo kukhulupirika kwa Yehova nʼkosatha.

Tamandani Yehova.

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 117:1-2

Zabbuli 117

1117:1 Bar 15:11*Mutendereze Mukama, mmwe ensi zonna;

mumugulumize, mmwe amawanga gonna.

2117:2 Zab 100:5Kubanga okwagala kwe okutaggwaawo kungi gye tuli;

n’obwesigwa bwa Mukama bwa lubeerera.

Mutendereze Mukama.