Masalimo 114 – CCL & HOF

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 114:1-8

Salimo 114

1Pamene Israeli anatuluka mu Igupto,

nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,

2Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu,

Israeli anasanduka ufumu wake.

3Nyanja inaona ndi kuthawa,

mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;

4mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna,

timapiri ngati ana ankhosa.

5Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa?

iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?

6inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna,

inu timapiri, ngati ana ankhosa?

7Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi,

pamaso pa Mulungu wa Yakobo,

8amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime,

thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.

Hoffnung für Alle

Psalm 114:1-8

Gott macht Geschichte

1Als Israel aus Ägypten zog,

als die Nachkommen von Jakob das Volk verließen,

das in einer fremden Sprache redete,

2da machte Gott das Gebiet Juda zu seinem Heiligtum

und Israel zu seinem Herrschaftsbereich.

3Das Schilfmeer sah ihn kommen und wich zurück,

auch der Jordan hörte auf zu fließen und staute sein Wasser.

4Die Berge sprangen wie die Schafböcke,

und die Hügel hüpften wie die Lämmer.

5Was ist mit dir geschehen, Meer?

Warum bist du so plötzlich zurückgewichen?

Jordan, warum hast du aufgehört zu fließen?

6Ihr Berge, weshalb seid ihr gesprungen wie die Schafböcke,

und ihr Hügel, warum seid ihr wie die Lämmer gehüpft?

7Erde, erbebe, wenn der Herr,

der Gott Jakobs, erscheint!

8Er verwandelte Felsen in Teiche voller Wasser

und ließ Quellen sprudeln, wo vorher nur harter Stein war!