Masalimo 112 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 112:1-10

Salimo 112

1Tamandani Yehova.

Wodala munthu amene amaopa Yehova,

amene amakondwera kwambiri ndi malamulo ake.

2Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko;

mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa.

3Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake,

ndipo chilungamo chake ndi chosatha.

4Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima;

wokoma mtima, wachifundo ndi wowongoka mtima.

5Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu,

amene amachita ntchito yake mwachilungamo.

6Ndithu sadzagwedezeka;

munthu wolungama sadzayiwalika mpaka muyaya.

7Saopa akamva zoyipa zimene zachitika;

mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.

8Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha;

potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano.

9Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka,

chilungamo chake chimanka mpaka muyaya;

nyanga yake idzakwezedwa mwaulemu.

10Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima;

adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka.

Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 112:1-10

Zabbuli 112

1112:1 a Zab 128:1 b Zab 119:14, 16, 47, 92Mutendereze Mukama!112:1 Mu Lwebbulaniya Aleruuya

Alina omukisa omuntu atya Katonda,

era asanyukira ennyo mu mateeka ge.

2Abaana be baliba ba kitiibwa mu nsi;

omulembe gw’abalongoofu guliweebwa omukisa.

3Ennyumba ye enejjulanga ebintu n’obugagga obungi;

era anaabanga mutuukirivu ennaku zonna.

4112:4 a Yob 11:17 b Zab 97:11Ne mu kizikiza, ekitangaala kyakira omulongoofu,

alina ekisa, n’oyo alina okusaasira, era omutuukirivu.

5112:5 Zab 37:21, 26Omuntu oyo agabira abeetaaga, era tawolera magoba,

era akola emirimu gye gyonna n’obwenkanya, alifuna ebirungi.

6112:6 Nge 10:7Omutuukirivu talinyeenyezebwa,

era anajjukirwanga ennaku zonna.

7112:7 Zab 57:7; Nge 1:33Amawulire amabi tegaamutiisenga,

kubanga omutima gwe munywevu gwesiga Mukama.

8112:8 Zab 59:10Omutima gwe guteredde, tewali ky’anaatyanga,

era oluvannyuma alitunuulira abalabe be n’amaaso ag’obuwanguzi.

9112:9 a 2Ko 9:9* b Zab 75:10Agabidde abaavu bye beetaaga;

mutuukirivu ebbanga lyonna;

era bonna banaamussangamu ekitiibwa.

10112:10 a Zab 86:17 b Zab 37:12 c Zab 58:7-8 d Nge 11:7Omubi anaabirabanga ebyo, n’asunguwala,

n’aluma abugigi, naye nga talina kya kukola.

Okwegomba kw’ababi tekuubengako kye kubagasa.