Masalimo 11 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 11:1-7

Salimo 11

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

1Mwa Yehova ine ndimathawiramo.

Nanga mungathe bwanji kunena kwa ine kuti,

“Thawira ku phiri lako ngati mbalame.

2Pakuti taona oyipa akunga mauta awo;

ayika bwino mivi yawo pa zingwe za uta,

pobisala pawo kuti alase

olungama mtima.

3Tsono ngati maziko awonongeka,

olungama angachite chiyani?”

4Yehova ali mʼNyumba yake yoyera;

Yehova ali pa mpando wake waufumu kumwamba.

Iye amayangʼanitsitsa ana a anthu;

maso ake amawayesa.

5Yehova amayesa olungama,

koma moyo wake umadana ndi oyipa,

amene amakonda zachiwawa.

6Iye adzakhuthulira pa oyipa

makala amoto ndi sulufule woyaka;

mphepo yotentha idzakhala yowayenera.

7Pakuti Yehova ndi wolungama,

Iye amakonda chilungamo;

ndipo anthu olungama adzaona nkhope yake.

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 11:1-7

Zabbuli 11

Ya Mukulu wa Bayimbi. Zabbuli ya Dawudi.

111:1 Zab 56:11Mu Mukama mwe neekweka;

ate muyinza mutya okuŋŋamba nti,

“Ddukira ku nsozi ng’ebinyonyi?

211:2 a Zab 7:13 b Zab 64:3-4Kubanga laba ababi baleega emitego gyabwe

egy’obusaale,

balase abalina omutima

omulongoofu.

311:3 Zab 82:5Emisingi nga gizikirizibwa,

omutuukirivu ayinza kukola ki?”

411:4 a Zab 18:6 b Zab 103:19 c Zab 33:13 d Zab 34:15-16Mukama ali mu Yeekaalu ye entukuvu;

Mukama atudde ku ntebe ye ey’obwakabaka eri mu ggulu.

Amaaso ge gatunuulira

era geetegereza abaana b’abantu.

511:5 a Lub 22:1; Yak 1:12 b Zab 5:5Mukama akebera abatuukirivu

naye omutima gwe gukyawa ababi,

n’abakola eby’obukambwe.

611:6 a Ez 38:22 b Yer 4:11-12Ababi alibayiwako

amanda ag’omuliro;

n’empewo ezibambula gwe guliba omugabo gwabwe.

711:7 a Zab 7:9, 11; 45:7 b Zab 33:5 c Zab 17:15Kubanga Mukama mutuukirivu

era ayagala eby’obutuukirivu;

abo abalongoofu be balimulaba.