Masalimo 100 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 100:1-5

Salimo 100

Salimo. Nyimbo yothokoza.

1Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.

2Mulambireni Yehova mosangalala;

bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.

3Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.

Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake;

ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.

4Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko

ndi ku mabwalo ake ndi matamando;

muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.

5Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;

kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 100:1-5

Zabbuli 100

Zabbuli ey’okwebaza.

1100:1 Zab 98:4Muleetere Mukama eddoboozi ery’essanyu mmwe ensi zonna.

2100:2 Zab 95:2Muweereze Mukama n’essanyu;

mujje mu maaso ge n’ennyimba ez’essanyu.

3100:3 a Zab 46:10 b Yob 10:3 c Zab 74:1; Ez 34:31Mumanye nga Mukama ye Katonda;

ye yatutonda, tuli babe,

tuli bantu be era endiga ez’omu ddundiro lye.

4100:4 Zab 116:17Muyingire mu miryango gye nga mwebaza,

ne mu mpya ze n’okutendereza;

mumwebaze mutendereze erinnya lye.

5100:5 a 1By 16:34; Zab 25:8 b Ezr 3:11; Zab 106:1 c Zab 119:90Kubanga Mukama mulungi, n’okwagala kwe kwa lubeerera;

n’obwesigwa bwe bwa mirembe gyonna.