BUKU LOYAMBA
Masalimo 1–41
Salimo 1
1Wodala munthu
amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa,
kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa,
kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
2Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova
ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
3Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi,
umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake
ndipo masamba ake safota.
Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
4Sizitero ndi anthu oyipa!
Iwo ali ngati mungu
umene umawuluzidwa ndi mphepo.
5Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo,
kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
6Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama,
koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.
Книга 1
Псалом 1
1Блажен человек,
который не следует совету нечестивых,
не стоит на пути грешников
и не сидит в собрании насмехающихся,
2но в Господнем Законе находит радость
и о Законе Его размышляет день и ночь.
3Он как дерево, посаженное у потоков вод,
которое приносит плод в свое время,
и чей лист не вянет.
Что бы он ни сделал, во всем преуспеет.
4Не таковы нечестивые!
Они как мякина,
которую гонит ветер.
5Поэтому не устоят на суде нечестивые,
и грешники – в собрании праведных.
6Ведь Господь охраняет путь праведных,
а путь нечестивых погибнет.