BUKU LOYAMBA
Masalimo 1–41
Salimo 1
1Wodala munthu
amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa,
kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa,
kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
2Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova
ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
3Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi,
umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake
ndipo masamba ake safota.
Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
4Sizitero ndi anthu oyipa!
Iwo ali ngati mungu
umene umawuluzidwa ndi mphepo.
5Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo,
kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
6Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama,
koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.
Первая книга
Песнь 1
1Благословен человек,
который не следует совету нечестивых,
не ходит путями грешников
и не сидит в собрании насмешников,
2но в Законе Вечного1:2 Вечный – на языке оригинала: «Яхве». Под этим именем Всевышний открылся Мусе и народу Исраила (см. Исх. 3:13-15). См. пояснительный словарь. находит радость
и о Законе Его размышляет день и ночь.
3Он как дерево, посаженное у потоков вод,
которое приносит плод в своё время,
и чей лист не вянет.
Что бы он ни сделал, во всём преуспеет.
4Не таковы нечестивые!
Они как мякина,
которую гонит ветер.
5Поэтому не устоят на суде нечестивые,
и грешники – в собрании праведных.
6Ведь Вечный охраняет путь праведных,
а путь нечестивых погибнет.