Hoseya 9 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Hoseya 9:1-17

Chilango cha Israeli

1Iwe Israeli, usakondwere;

monga imachitira mitundu ina.

Pakuti wakhala wosakhulupirika kwa Mulungu wako;

umakonda malipiro a chiwerewere

pa malo aliwonse opunthira tirigu.

2Malo opunthira tirigu ndi malo opsinyira mphesa sadzadyetsa anthu;

adzasowa vinyo watsopano.

3Sadzakhalanso mʼdziko la Yehova.

Efereimu adzabwerera ku Igupto

ndipo mudzadya chakudya chodetsedwa ku Asiriya.

4Iwo sadzaperekanso chopereka cha chakumwa kwa Yehova,

kapena nsembe zawo kuti akondweretse Yehovayo.

Nsembe zotere zidzakhala kwa iwo ngati chakudya cha anamfedwa;

onse akudya chakudya chimenechi adzakhala odetsedwa.

Chakudya ichi chidzakhala chodya okha,

sichidzalowa mʼnyumba ya Yehova.

5Kodi mudzachita chiyani pa tsiku la maphwando anu oyikika;

pa masiku a zikondwerero za Yehova?

6Ngakhale iwo atathawa chiwonongeko,

Igupto adzawasonkhanitsa,

ndipo Mefisi adzawayika mʼmanda.

Khwisa adzamera pa ziwiya zawo zasiliva,

ndipo minga idzamera mʼmatenti awo.

7Masiku achilango akubwera,

masiku obwezera ali pafupi.

Israeli adziwe zimenezi.

Chifukwa machimo anu ndi ochuluka kwambiri

ndipo udani wanu pa Mulungu ndi waukulu kwambiri.

Mneneri amamuyesa chitsiru,

munthu wanzeru za kwa Mulungu ngati wamisala.

8Mneneri pamodzi ndi Mulungu wanga

ndiwo alonda a Efereimu,

koma mneneri amutchera misampha mʼnjira zake zonse,

ndipo udani ukumudikira mʼnyumba ya Mulungu wake.

9Iwo azama mu zachinyengo

monga masiku a Gibeya.

Mulungu adzakumbukira zolakwa zawo

ndipo adzawalanga chifukwa cha machimo awo.

10“Pamene ndinamupeza Israeli

zinali ngati kupeza mphesa mʼchipululu.

Nditaona makolo anu,

zinali ngati ndikuona nkhuyu zoyambirira kupsa.

Koma atafika ku Baala Peori,

anadzipereka ku fano lija lochititsa manyazi

ndipo anakhala onyansa ngati chinthu chimene anachikondacho.

11Ulemerero wa Efereimu udzawuluka ngati mbalame.

Sipadzakhalanso kubereka ana, kuyembekezera kapena kutenga pathupi.

12Ngakhale atalera ana

ndidzachititsa kuti mwana aliyense amwalire.

Tsoka kwa anthuwo

pamene Ine ndidzawafulatira!

13Ndaona Efereimu ngati Turo,

atadzalidwa pa nthaka ya chonde.

Koma Efereimu adzatsogolera

ana ake kuti akaphedwe.”

14Inu Yehova, muwapatse.

Kodi mudzawapatsa chiyani?

Apatseni mimba yomangopita padera

ndi mawere owuma.

15“Chifukwa cha zoyipa zawo zonse ku Giligala,

Ine ndinawada kumeneko.

Chifukwa cha machitidwe awo auchimo,

ndidzawapirikitsa mʼnyumba yanga.

Sindidzawakondanso;

atsogoleri awo onse ndi owukira.

16Efereimu wathedwa,

mizu yake yauma

sakubalanso zipatso.

Ngakhale atabereka ana,

Ine ndidzapha ana awo okondedwawo.”

17Mulungu wanga adzawakana

chifukwa sanamumvere Iye;

adzakhala oyendayenda pakati pa anthu a mitundu ina.

Luganda Contemporary Bible

Koseya 9:1-17

Okubonerezebwa kwa Isirayiri

19:1 a Is 22:12-13 b Kos 10:5Tosanyuka ggwe Isirayiri;

tojaguza ng’amawanga amalala,

kubanga tobadde mwesigwa eri Katonda wo,

weegomba empeera eya malaaya

ku buli gguuliro.

29:2 Kos 2:9Egguuliro n’essogolero tebiribaliisa,

ne wayini omusu alibaggwaako.

39:3 a Lv 25:23 b Kos 8:13 c Ez 4:13; Kos 7:11Tebalisigala mu nsi ya Mukama;

Efulayimu aliddayo e Misiri

n’alya emmere etali nnongoofu mu Bwasuli.

49:4 a Yer 6:20; Kos 8:13 b Kag 2:13-14Tebaliwaayo biweebwayo ebya wayini eri Mukama,

so ne ssaddaaka zaabwe tezirimusanyusa.

Ssaddaaka zaabwe ziriba ng’emmere ey’abakungubazi,

ne bonna abaliziryako balifuuka abatali balongoofu.

Emmere eyo eriba yaabwe bo,

so teriyingizibwa mu yeekaalu ya Mukama.

59:5 a Is 10:3; Yer 5:31 b Kos 2:11Kiki ky’olikola ku lunaku olw’embaga ezaalondebwa,

ku lunaku olw’embaga ya Mukama?

69:6 a Is 19:13 b Is 5:6; Kos 10:8Ne bwe baliwona okuzikirira,

Misiri alibakuŋŋaanya,

ne Menfisi alibaziika.

Eby’obugagga byabwe ebya ffeeza birizika,

n’eweema zaabwe zirimeramu amaggwa.

79:7 a Is 34:8; Yer 10:15; Mi 7:4 b Yer 16:18 c Is 44:25; Kgb 2:14; Ez 14:9-10Ennaku ez’okubonerezebwa zijja,

ennaku ez’okusasulirwamu ziri kumpi.

Ekyo Isirayiri akimanye.

Olw’ebibi byammwe okuba ebingi ennyo,

n’obukambwe bwammwe obungi,

nnabbi ayitibwa musirusiru,

n’oyo eyabikkulirwa mumuyita mugu wa ddalu.

89:8 Kos 5:1Nnabbi awamu ne Katonda wange

ye mukuumi wa Efulayimu,9:8 Efulayimu be bantu ba Katonda

newaakubadde nga waliwo emitego mu kkubo lye,

n’obukambwe mu nnyumba ya Katonda we.

99:9 a Bal 19:16-30; Kos 5:8; 10:9 b Kos 8:13Boonoonye nnyo nnyini

nga mu nnaku ez’e Gibea.

Katonda alijjukira obutali butuukirivu bwabwe,

n’ababonereza olw’ebibi byabwe.

109:10 a Kbl 25:1-5; Zab 106:28-29 b Yer 11:13; Kos 4:14We nasangira Isirayiri,

kyali nga kulaba zabbibu mu ddungu.

Bwe nalaba bajjajjammwe,

kyali nga kulaba ebibala ebisooka ku mutiini.

Naye bwe bajja e Baalipyoli,

beewonga eri ekifaananyi eky’ensonyi,

ne bafuuka ekyenyinnyalwa ng’ekifaananyi kye baayagala.

119:11 a Kos 4:7; 10:5 b nny 14Ekitiibwa kya Efulayimu kiribuuka ne kigenda ng’ekinyonyi

nga tewali kuzaala, newaakubadde okuba olubuto newaakubadde okufuna olubuto.

129:12 a Kos 7:13 b Ma 31:17Ne bwe balikuza abaana baabwe,

ndibabaggyako bonna.

Ziribasanga

bwe ndibavaako.

139:13 Ez 27:3Nalaba Efulayimu

ng’asimbiddwa mu kifo ekirungi, nga Ttuulo bw’ali.

Naye Efulayimu alifulumya

abaana be ne battibwa.

149:14 nny 11; Luk 23:29Bawe Ayi Mukama Katonda.

Olibawa ki?

Leetera embuto zaabwe okuvaamu

obawe n’amabeere amakalu.

159:15 a Kos 4:15 b Kos 7:2 c Is 1:23; Kos 4:9; 5:2Olw’ebibi byabwe byonna mu Girugaali,

kyennava mbakyayira eyo.

Olw’ebikolwa byabwe ebitali bya butuukirivu,

kyendiva mbagoba mu nnyumba yange.

Siribaagala nate;

abakulembeze baabwe bonna bajeemu.

169:16 a Kos 5:11 b Kos 8:7 c nny 12Efulayimu balwadde,

emirandira gyabwe gikaze,

tebakyabala bibala.

Ne bwe balizaala abaana baabwe,

nditta ezzadde lyabwe lye baagala ennyo.

179:17 a Kos 4:10 b Ma 28:65; Kos 7:13Katonda wange alibavaako

kubanga tebamugondedde;

baliba momboze mu mawanga.