Estere 10 – CCL & CCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Estere 10:1-3

Ukulu wa Mordekai

1Mfumu Ahasiwero anakhometsa msonkho mʼdziko lake lonse mpaka ku zilumba zonse. 2Ndipo ntchito zonse zochitika ndi mphamvu zake komanso ndi zonse zofotokoza za ukulu wa Mordekai, kukwezedwa kwake ndi mfumu, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Mediya ndi Peresiya? 3Pakuti Mordekai Myuda uja anali wachiwiri wa mfumu Ahasiwero. Kwa Ayuda onse Mordekai anali munthu wamkulu ndipo ankamukonda chifukwa ankachitira zabwino mtundu wake ndi kufunira mtendere abale ake.

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

以斯帖记 10:1-3

亚哈随鲁和末底改的功绩

1亚哈随鲁王使内陆和沿海的人民都进贡。 2他所有的丰功伟绩以及擢升末底改的事都记在玛代波斯的史书上。 3犹太末底改的地位仅次于亚哈随鲁王,他在犹太人中受尊崇,得到同胞的爱戴,因为他致力于本族人的益处,为他们谋求福祉。