Estere 10 – CCL & CARST

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Estere 10:1-3

Ukulu wa Mordekai

1Mfumu Ahasiwero anakhometsa msonkho mʼdziko lake lonse mpaka ku zilumba zonse. 2Ndipo ntchito zonse zochitika ndi mphamvu zake komanso ndi zonse zofotokoza za ukulu wa Mordekai, kukwezedwa kwake ndi mfumu, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Mediya ndi Peresiya? 3Pakuti Mordekai Myuda uja anali wachiwiri wa mfumu Ahasiwero. Kwa Ayuda onse Mordekai anali munthu wamkulu ndipo ankamukonda chifukwa ankachitira zabwino mtundu wake ndi kufunira mtendere abale ake.

Священное Писание (Восточный перевод), версия для Таджикистана

Есфирь 10:1-3

Величие Мардохея

1Царь Ксеркс наложил дань на всё царство до самых далёких его побережий. 2Все дела его власти и могущества и полный рассказ о величии Мардохея, которым наделил его царь, записаны в «Летописи царей Мидии и Персии». 3Иудей Мардохей был вторым после царя Ксеркса; он был велик среди иудеев, и множество соплеменников глубоко чтило его, потому что он трудился на благо своего народа и говорил ради благополучия всех иудеев.