2 Akorinto 13 – CCL & CARSA

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Akorinto 13:1-14

Mawu Otsiriza ndi Ochenjeza

1Uwu ndi ulendo wachitatu ndikubwera kudzakuyenderani. “Nkhani itsimikizike ndi umboni wa anthu awiri kapena atatu.” 2Ndinakuchenjezani kale pamene ndinali nanu ulendo wachiwiri uja. Tsopano ndikubwereza ndisanafike. Ndikabweranso sindidzachitira chifundo amene anachimwa poyamba paja kapena wina aliyense amene anachimwa, 3popeza mufuna chitsimikizo chakuti Khristu akuyankhula kudzera mwa ine. Iye siwofowoka pofuna kuchita nanu koma ndi wamphamvu pakati panu. 4Pofuna kutsimikizira, anapachikidwa ali wofowoka koma ali ndi moyo mwamphamvu ya Mulungu. Chomwechonso, ife ndife ofowoka mwa Iye, koma tidzakhala ndi moyo pamodzi naye ndi mphamvu ya Mulungu, potumikira pakati panu.

5Tadzisanthulani nokha kuti muone ngati muli mʼchikhulupiriro; dziyeseni nokha. Kodi simuzindikira kuti Khristu Yesu ali mwa inu, ngati si choncho mwalephera mayesowa? 6Ndipo ndikhulupirira kuti mudzazindikira kuti ife sitinalephere mayesowo. 7Tsopano tikupemphera kwa Mulungu kuti musadzachite kanthu kena kalikonse kolakwa. Osati chifukwa choti anthu aone kuti ife tapambana mayesowo koma kuti mudzachite zokhoza ngakhale anthu atamationa ngati olephera. 8Pakuti sitingachite chilichonse chotsutsana ndi choonadi, koma chokhacho chovomerezana ndi choonadi. 9Ife timasangalala kuti pamene tafowoka, inu muli amphamvu; ndipo pemphero lathu ndi lakuti mukhale angwiro. 10Nʼchifukwa chake ndimalemba zinthu zoterezi pamene ndili kutali, kuti ndikabwera ndisadzagwiritse ntchito ulamuliro wanga mokalipa, uwu ndi ulamuliro umene Ambuye anandipatsa kuti ndikukuzeni inu osati kukuwonongani.

Malonje Otsiriza

11Potsiriza abale, ndikuti tsalani bwino. Yesetsani kukhala angwiro, mvetsetsani pempho langa, khalani a mtima umodzi, khalani mwamtendere. Ndipo Mulungu wachikondi ndi mtendere adzakhala nanu.

12Lonjeranani ndi mpsopsono wachiyero. 13Anthu onse a Mulungu akupereka moni.

14Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu, ndi chikondi cha Mulungu, ndi chiyanjano cha Mzimu Woyera zikhale ndi inu nonse.

Священное Писание (Восточный перевод), версия с «Аллахом»

2 Коринфянам 13:1-13

Заключительные предостережения

1Я прихожу к вам в третий раз. Помните, что «любое обвинение должно подтверждаться показаниями двух или трёх свидетелей»13:1 Втор. 19:15.. 2Я уже предупреждал вас, когда был у вас во второй раз, и сейчас, находясь вдали, я повторяю это всем, кто согрешил прежде, да и всем остальным: в этот раз я жалеть вас не буду. 3Вы хотите видеть доказательство того, что через меня говорит аль-Масих? Его сила не ослабла, и Он проявляет её среди вас! 4И хотя аль-Масих был распят в слабости, но Он жив могуществом Аллаха! И мы, находясь в единении с Ним, также слабы, но будем жить с Ним могуществом Аллаха, чтобы служить вам.

5Проверяйте себя, в вере ли вы; испытывайте себя. Неужели вы не знаете, что в вас живёт Иса аль-Масих?13:5 То, что в верующих коринфянах живёт Повелитель Иса, само по себе доказывает, что через Паула говорит Иса аль-Масих (см. ст. 3), так как они пришли к вере в аль-Масиха через служение Паула. Если, конечно, вы выдержали это испытание. 6А что касается нас, то, я надеюсь, вы увидите, что мы испытание выдержали. 7Мы молимся Аллаху о том, чтобы вы не сделали зла. Не ради того, чтобы нам выглядеть выдержавшими испытание, а ради того, чтобы вы поступали по правде, пусть даже мы и не будем казаться выдержавшими. 8Мы не можем делать ничего вопреки истине, а только ради истины.

9Мы даже рады быть слабыми, если вы будете действительно сильны, и мы молимся о том, чтобы вы шли к исправлению. 10Находясь сейчас не с вами, я пишу вам для того, чтобы, когда я буду у вас, мне не пришлось бы проявлять строгости. Повелитель дал мне власть не для того, чтобы разрушать, а для того, чтобы созидать.

Заключительные приветствия

11И в заключение, братья, хочу сказать: радуйтесь, стремитесь к исправлению, ободряйте друг друга13:11 Или: «примите мои наставления»., пусть среди вас будет единство, живите в мире, и Аллах, источник любви и мира, будет с вами.

12Приветствуйте друг друга святым поцелуем13:12 Поцелуем приветствовали и приветствуют доныне друг друга жители Ближнего Востока. Подобное можно наблюдать и в Центральной Азии.. Вас приветствует весь святой народ Аллаха.

13Пусть со всеми вами будет благодать Повелителя Исы аль-Масиха, любовь Аллаха и общение Святого Духа.