1 Mbiri 27 – CCL & NRT

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mbiri 27:1-34

Magulu a Anthu Ankhondo

1Uwu ndi mndandanda wa Aisraeli, atsogoleri a mabanja, olamulira asilikali 1,000, olamulira asilikali 100 ndi akuluakulu awo, amene ankatumikira mfumu mʼzonse zokhudza magulu a ankhondo, amene amagwira ntchito mwezi ndi mwezi chaka chonse. Gulu lililonse linali ndi anthu 24,000.

2Amene amalamulira gulu loyamba pa mwezi woyamba anali Yasobeamu mwana wa Zabidieli. Pa gulu lake panali asilikali 24,000. 3Iyeyu anali chidzukulu cha Perezi ndipo anali mkulu wa atsogoleri onse a ankhondo mwezi woyamba.

4Amene amalamulira gulu lachiwiri pa mwezi wachiwiri anali Dodai Mwahohi; Mikiloti ndiye anali mtsogoleri wa gulu lake. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

5Wolamulira ankhondo wachitatu, pa mwezi wachitatu anali Benaya, mwana wa wansembe Yehoyada. Iye anali mtsogoleri ndipo pa gulu lake panali ankhondo 24,000. 6Uyu ndi Benaya uja amene anali wamphamvu pa gulu la anthu makumi atatu ndipo ndiye amatsogolera anthu makumi atatu aja. Mwana wake Amizabadi ndiye amatsogolera gulu lake.

7Wachinayi pa mwezi wachinayi anali Asaheli mʼbale wake wa Yowabu; ndipo mwana wake Zebadiya ndiye analowa mʼmalo mwake. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

8Wachisanu pa mwezi wachisanu anali Samihuti, mdzukulu wa Izira. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

9Wa 6 pa mwezi wa 6 anali Ira mwana wa Ikesi wa ku Tekowa. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

10Wa 7 pa mwezi wa 7 anali Helezi Mpeloni wa fuko la Efereimu. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

11Wa 8 pa mwezi wa 8 anali Sibekai Mhusati, wa mbumba ya Zera. Pa gulu lake panali asilikali 24,000

12Wa 9 pa mwezi wa 9 anali Abiezeri wa banja la Anatoti, wa fuko la Benjamini. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

13Wa khumi pa mwezi wa khumi anali Mahazayi wa ku Netofa, wa mbumba ya Zera. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

14Mtsogoleri wa 11, pa mwezi wa 11 anali Benaya wa ku Piratoni, wa fuko la Efereimu. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

15Mtsogoleri wa 12, pa mwezi wa 12 anali Helidai Mnetofa, wa banja la Otanieli. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.

Akuluakulu a Mafuko a Israeli

16Akuluakulu amene amatsogolera mafuko a Israeli ndi awa:

Mtsogoleri wa fuko la Rubeni: Eliezara mwana wa Zikiri;

mtsogoleri wa fuko la Simeoni: Sefatiya mwana wa Maaka;

17mtsogoleri wa fuko la Levi: Hasabiya mwana wa Kemueli,

mtsogoleri wa banja la Aaroni: Zadoki;

18mtsogoleri wa fuko la Yuda: Elihu, mʼbale wake wa Davide;

mtsogoleri wa fuko la Isakara: Omuri mwana wa Mikayeli;

19mtsogoleri wa fuko la Zebuloni: Isimaiya mwana wa Obadiya;

mtsogoleri wa fuko la Nafutali: Yerimoti mwana wa Azirieli;

20mtsogoleri wa fuko la Efereimu: Hoseya mwana wa Azaziya;

mtsogoleri wa fuko la theka la Manase: Yoweli mwana wa Pedaya;

21mtsogoleri wa fuko la theka la Manase limene linali ku Giliyadi: Ido mwana wa Zekariya;

mtsogoleri wa fuko la Benjamini: Yaasieli mwana wa Abineri;

22mtsogoleri wa fuko la Dani: Azareli mwana wa Yerohamu.

Awa anali akuluakulu a mafuko a Israeli.

23Davide sanawerenge amuna amene anali ndi zaka makumi awiri kapena kucheperapo, chifukwa Yehova analonjeza kuti adzachulukitsa Aisraeli ngati nyenyezi zamumlengalenga. 24Yowabu mwana wa Zeruya anayamba kuwerenga amuna koma sanamalize. Mkwiyo unagwera Aisraeli chifukwa cha zimenezi ndipo chiwerengerochi sanachilowetse mʼbuku la mbiri ya mfumu Davide.

Anthu Oyangʼanira Chuma cha Mfumu

25Azimaveti mwana wa Adieli ankayangʼanira nyumba zosungiramo katundu wa mfumu.

Yonatani mwana wa Uziya ankayangʼanira nyumba zosungiramo katundu wa maboma ozungulira, mizinda, midzi ndi malo olondera.

26Eziri mwana wa Kelubi ankayangʼanira anthu ogwira ntchito yolima ku munda.

27Simei wa ku Rama ankayangʼanira minda ya mpesa.

Zabidi wa ku Sifamu ankayangʼanira mphesa ndi mosungiramo mwake.

28Baala-Hanani wa ku Gederi ankayangʼanira mitengo ya olivi ndi ya mikuyu ya ku Sefela.

Yowasi ankayangʼanira mafuta a Olivi.

29Sitirayi wa ku Saroni ankayangʼanira ziweto zimene amaweta ku Saroni.

Safati mwana wa Adilayi ankayangʼanira ngʼombe zakuzigwa.

30Obili Mwismaeli ankayangʼanira ngamira.

Yehideya Mmerenoti ankayangʼanira abulu.

31Yazizi Mhagiri akayangʼanira nkhosa ndi mbuzi.

Onsewa anali akuluakulu oyangʼanira chuma cha mfumu Davide.

32Yonatani, malume wake wa Davide, anali phungu wake ndipo anali munthu wanzeru komanso analinso mlembi. Yehieli mwana wa Hakimoni ankasamalira ana a mfumu.

33Ahitofele anali phungu wa mfumu.

Husai Mwariki anali bwenzi la mfumu. 34Ahitofele atamwalira mʼmalo mwake munalowa Yehoyada mwana wa Benaya ndi Abiatara.

Yowabu anali mtsogoleri wa gulu lankhondo la mfumu.

New Russian Translation

1 Паралипоменон 27:1-34

Войсковое деление

1Вот перечень израильтян – глав семейств, тысячников, и сотников, и их чиновников, которые служили царю во всем, что относилось к войсковым отделениям, несшим службу по месяцу в течение года. В каждом отделении было двадцать четыре тысячи воинов.

2Во главе первого отделения для первого месяца стоял Иашовеам, сын Завдиила. В его отделении было двадцать четыре тысячи воинов. 3Он был потомком Пареца и главой всех военачальников в первый месяц.

4Во главе отделения для второго месяца стоял ахохитянин Додай; его главным воеводой был Миклот. В его отделении было двадцать четыре тысячи воинов.

5Третьим военачальником для третьего месяца был Беная, сын священника Иодая. Он был вождем, и в его отделении было двадцать четыре тысячи воинов. 6Это тот Беная, который был могучим воином среди тех тридцати и начальником над ними. Его сын Аммизавад стоял над его отделением.

7Четвертым для четвертого месяца был Асаил, брат Иоава; его сын Зевадия был его преемником. В его отделении было двадцать четыре тысячи воинов.

8Пятым для пятого месяца был военачальник Шамгут27:8 Шамгут – вариант имени Шамма (см. 11:27 и 2 Цар. 23:25). израхитянин. В его отделении было двадцать четыре тысячи воинов.

9Шестым для шестого месяца был Ира, сын текоитянина Иккеша. В его отделении было двадцать четыре тысячи воинов.

10Седьмым для седьмого месяца был пелонитянин Хелец из потомков Ефрема. В его отделении было двадцать четыре тысячи воинов.

11Восьмым для восьмого месяца был хушатянин Сивхай, потомок Зераха. В его отделении было двадцать четыре тысячи воинов.

12Девятым для девятого месяца был анатотянин Авиезер из потомков Вениамина. В его отделении было двадцать четыре тысячи воинов.

13Десятым для десятого месяца был нетофитянин Магарай, потомок Зераха. В его отделении было двадцать четыре тысячи воинов.

14Одиннадцатым для одиннадцатого месяца был пирафонянин Беная из потомков Ефрема. В его отделении было двадцать четыре тысячи человек.

15Двенадцатым для двенадцатого месяца был нетофитянин Хелдай, потомок Отниила. В его отделении было двадцать четыре тысячи человек.

Вожди израильских родов

16Вождями родов Израиля были:

у Рувима: Элиезер, сын Зихрия;

у Симеона: Шефатия, сын Маахи;

17у Левия: Хашавия, сын Кемуила;

у Аарона: Цадок;

18у Иуды: Элигу, брат Давида;

у Иссахара: Омри, сын Михаила;

19у Завулона: Ишмая, сын Авдия;

у Неффалима: Иеримот, сын Азриила;

20у Ефрема: Осия, сын Азазии;

у половины рода Манассии: Иоиль, сын Педаи;

21у половины рода Манассии в Галааде: Иддо, сын Захарии;

у Вениамина: Иаасиил, сын Авнера;

22у Дана: Азариил, сын Иерохама.

Это вожди родов Израиля.

23Давид не считал тех, кому было двадцать лет или меньше, потому что Господь обещал сделать Израиль многочисленным, как звезды на небе. 24Иоав, сын Саруи, начал пересчитывать народ, но не закончил: гнев за эту перепись постиг Израиль, и ее результат не был вписан в «Летопись царя Давида».

Царские сановники

25Азмавету, сыну Адиила, было поручено смотреть за царскими кладовыми.

Ионафану, сыну Уззии, за кладовыми в провинции: в городах, поселениях и сторожевых башнях.

26Езрию, сыну Хелува, за работниками на поле, которые возделывали землю.

27Раматитянину Шимею – за виноградниками.

Шифмитянину Завдию – за запасами вина в винных погребах.

28Гедеритянину Баал-Ханану – за оливковыми и тутовыми деревьями в западных предгорьях.

Иоашу – за запасами оливкового масла.

29Шаронитянину Шитраю – за крупным скотом, пасущемся в районе Шарон, а Шафату, сыну Адлая, за крупным скотом в долинах.

30Измаильтянину Овилу – за верблюдами.

Меронофянину Иехдии – за ослами.

31Агаритянину Иазизу – за мелким скотом.

Это сановники, которым было поручено смотреть за добром царя Давида.

Советники Давида

32Ионафан, дядя Давида, проницательный человек и писарь, был советником. Иехиил, сын Хахмония, воспитывал царских сыновей.

33Ахитофел был царским советником.

Аркитянин Хусий был другом царя. 34Преемниками Ахитофела были Иодай, сын Бенаи, и Авиатар.

Иоав стоял во главе царского войска.