1 Mbiri 25 – CCL & CST

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mbiri 25:1-31

Anthu Oyimba Nyimbo

1Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:

2Kuchokera kwa ana a Asafu:

Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.

3Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake:

Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.

4Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake:

Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti. 5Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.

6Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu. 7Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288. 8Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.

9Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe,    ana ndi abale ake. 12Maere achiwiri anagwera Gedaliya,    ndi abale ake ndi ana ake. 1210Maere achitatu anagwera Zakuri,    ana ake ndi abale ake.1211Maere achinayi anagwera Iziri,    ana ake ndi abale ake.1212Maere achisanu anagwera Netaniya,    ana ake ndi abale ake.1213Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya,    ana ake ndi abale ake.1214Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela,    ana ake ndi abale ake.1215Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya,    ana ake ndi abale ake.1216Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya,    ana ake ndi abale ake.1217Maere a khumi anagwera Simei,    ana ake ndi abale ake.1218Maere a 11 anagwera Azareli,    ana ake ndi abale ake.1219Maere a 12 anagwera Hasabiya,    ana ake ndi abale ake.1220Maere a 13 anagwera Subaeli,    ana ake ndi abale ake.1221Maere a 14 anagwera Matitiya,   ana ake ndi abale ake.1222Maere a 15 anagwera Yeremoti,   ana ake ndi abale ake.1223Maere a 16 anagwera Hananiya,   ana ake ndi abale ake.1224Maere a 17 anagwera Yosibakasa,   ana ake ndi abale ake.1225Maere a 18 anagwera Hanani,   ana ake ndi abale ake.1226Maere a 19 anagwera Maloti,   ana ake ndi abale ake.1227Maere a 20 anagwera Eliyata,   ana ake ndi abale ake.1228Maere a 21 anagwera Hotiri,   ana ake ndi abale ake.1229Maere a 22 anagwera Gidaliti,   ana ake ndi abale ake.1230Maere a 23 anagwera Mahazioti,   ana ake ndi abale ake.1231Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri,   ana ake ndi abale ake12.

Nueva Versión Internacional (Castilian)

1 Crónicas 25:1-31

Organización de los músicos

1Para el ministerio de la música, David y los comandantes del ejército apartaron a los hijos de Asaf, Hemán y Jedutún, los cuales profetizaban acompañándose de arpas, liras y címbalos. Esta es la lista de los que fueron apartados para el servicio:

2De los hijos de Asaf: Zacur, José, Netanías y Asarela. A estos los dirigía Asaf, quien profetizaba bajo las órdenes del rey.

3De Jedutún, sus seis hijos: Guedalías, Zeri, Isaías, Simí,25:3 Simí (un ms. hebreo y mss. de LXX); TM no incluye este nombre. Jasabías y Matatías. A estos los dirigía su padre Jedutún, quien al son del arpa profetizaba para dar gracias y alabar al Señor.

4De los hijos de Hemán: Buquías, Matanías, Uziel, Sebuel, Jeremot, Jananías, Jananí, Eliatá, Guidalti, Romanti Ezer, Josbecasa, Malotí, Hotir y Mahaziot. 5Todos estos fueron hijos de Hemán, vidente del rey, y con la palabra de Dios exaltaban su poder.25:5 su poder. Lit. el cuerno. Dios le dio a Hemán catorce hijos y tres hijas.

6Su padre los dirigía en el culto del templo del Señor, cuando cantaban acompañados de címbalos, liras y arpas. Asaf, Jedutún y Hemán estaban bajo las órdenes del rey. 7Ellos eran en total doscientos ochenta y ocho, incluyendo a sus demás compañeros, y habían sido instruidos para cantarle al Señor.

8Para asignarles sus turnos se echaron suertes, sin hacer distinción entre menores y mayores, ni entre maestros y discípulos.

9La primera suerte le tocó a José el asafita;

la segunda le tocó a Guedalías, junto con sus hermanos y sus hijos, doce en total.

10La tercera, a Zacur, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

11La cuarta, a Izri, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

12La quinta, a Netanías, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

13La sexta, a Buquías, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

14La séptima, a Jesarela, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

15La octava, a Isaías, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

16La novena, a Matanías, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

17La décima, a Simí, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

18La undécima, a Azarel, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

19La duodécima, a Jasabías, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

20La decimotercera, a Subael, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

21La decimocuarta, a Matatías, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

22La decimoquinta, a Jeremot, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

23La decimosexta, a Jananías, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

24La decimoséptima, a Josbecasa, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

25La decimoctava, a Jananí, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

26La decimonovena, a Malotí, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

27La vigésima, a Eliatá, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

28La vigesimoprimera, a Hotir, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

29La vigesimosegunda, a Guidalti, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

30La vigesimotercera, a Mahaziot, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.

31La vigesimocuarta, a Romanti Ezer, junto con sus hijos y hermanos, doce en total.