1 Mbiri 1 – CCL & JCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mbiri 1:1-54

Mbiri ya Makolo Kuchokera pa Adamu Mpaka pa Abrahamu

Mpaka pa Ana a Nowa

1Adamu, Seti, Enosi 2Kenani, Mahalaleli, Yaredi, 3Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.

4Ana a Nowa,

Semu, Hamu ndi Yafeti.

Fuko la Yafeti

5Ana aamuna a Yafeti anali:

Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.

6Ana aamuna a Gomeri anali:

Asikenazi, Rifati ndi Togarima

7Ana aamuna a Yavani anali:

Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.

Fuko la Hamu

8Ana aamuna a Hamu anali:

Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani

9Ana aamuna a Kusi anali:

Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka

Ana aamuna a Raama anali:

Seba ndi Dedani.

10Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu

kwambiri pa dziko lapansi.

11Igupto ndiye kholo la

Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu, 12Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.

13Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni,

ndipo anaberekanso Ahiti, 14Ayebusi, Aamori, Agirigasi 15Ahivi, Aariki, Asini 16Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.

Fuko la Semu

17Ana aamuna a Semu anali:

Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu.

Ana aamuna a Aramu anali:

Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.

18Aripakisadi anabereka Sela

ndipo Selayo anabereka Eberi:

19Eberi anabereka ana aamuna awiri:

wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.

20Yokitani anabereka

Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera, 21Hadoramu, Uzali, Dikila 22Obali, Abimaeli, Seba, 23Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.

24Semu, Aripakisadi, Sela

25Eberi, Pelegi, Reu

26Serugi, Nahori, Tera

27ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).

Banja la Abrahamu

28Ana a Abrahamu ndi awa:

Isake ndi Ismaeli.

Zidzukulu za Hagara

29Zidzukulu zake zinali izi:

Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu, 30Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema, 31Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.

Zidzukulu za Ketura

32Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa:

Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa.

Ana a Yokisani ndi awa:

Seba ndi Dedani

33Ana aamuna a Midiyani anali,

Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida.

Onsewa anali zidzukulu za Ketura.

Zidzukulu za Sara

34Abrahamu anabereka Isake.

Ana a Isake anali awa:

Esau ndi Israeli.

Ana a Esau

35Ana aamuna a Esau anali awa:

Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.

36Ana a Elifazi anali awa:

Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi:

Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.

37Ana a Reueli anali awa:

Nahati, Zera, Sama ndi Miza.

Anthu a ku Seiri ku Edomu

38Ana a Seiri anali awa:

Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.

39Ana aamuna a Lotani anali awa:

Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.

40Ana aamuna a Sobala anali awa:

Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu.

Ana aamuna a Zibeoni anali awa:

Ayiwa ndi Ana.

41Mwana wa Ana anali

Disoni.

Ana a Disoni anali awa:

Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani

42Ana aamuna a Ezeri anali awa:

Bilihani, Zaavani ndi Yaakani.

Ana aamuna a Disani anali awa:

Uzi ndi Arani.

Mafumu a ku Edomu

43Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko:

Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.

44Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.

45Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.

46Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.

47Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.

48Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.

49Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.

50Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu. 51Hadadi anamwaliranso.

Mafumu a ku Edomu anali:

Timna, Aliva, Yeteti, 52Oholibama, Ela, Pinoni, 53Kenazi, Temani, Mibezari, 54Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.

Japanese Contemporary Bible

歴代誌Ⅰ 1:1-54

1

アダムからアブラハムまでの系図

1-4人類の最初の先祖は、次のとおりです。

アダム、セツ、エノシュ、ケナン、マハラルエル、エレデ、エノク、メトシェラ、レメク、ノア、セム、ハム、ヤペテ。

5-9ヤペテの子孫はゴメル、マゴグ、マダイ、ヤワン、トバル、メシェク、ティラス。

ゴメルの子孫はアシュケナズ、ディファテ、トガルマ。

ヤワンの子孫はエリシャ、タルシシュ、キティム、ロダニム。

ハムの子孫はクシュ、ミツライム、プテ、カナン。

クシュの子孫はセバ、ハビラ、サブタ、ラマ、サブテカ。

ラマの子孫はシェバ、デダン。

10クシュのもう一人の子ニムロデは、偉大な英雄でした。

11-12ミツライムの子孫の名をとって呼ばれる氏族は、次のとおり。ルデ人、アナミム人、レハビム人、ナフトヒム人、パテロス人、ペリシテ人の先祖カスルヒム人、カフトル人。

13-16カナンの息子は長男のシドンとヘテ。

カナンは、エブス人、エモリ人、ギルガシ人、ヒビ人、アルキ人、シニ人、アルワデ人、ツェマリ人、ハマテ人の先祖となりました。

17セムの子孫はエラム、アシュル、アルパクシャデ、ルデ、アラム、ウツ、フル、ゲテル、メシェク。

18アルパクシャデの子はシェラフ、シェラフの子はエベル。

19エベルの息子は、「分割」という意味のペレグ。彼の時代に、地上の人々が異なる言語ごとに分けられたからです。そして、もう一人はヨクタン。

20-23ヨクタンの子孫はアルモダデ、シェレフ、ハツァルマベテ、エラフ、ハドラム、ウザル、ディクラ、エバル、アビマエル、シェバ、オフィル、ハビラ、ヨバブ。

24-27こういうわけで、セムの子はアルパクシャデ、その子はシェラフ。以下、エベル、ペレグ、レウ、セルグ、ナホル、テラ、アブラム(のちにアブラハムと改名)と続きます。

アブラハムの子孫

28-31アブラハムの子はイサクとイシュマエル。

イシュマエルの子孫は次のとおり。長男ネバヨテ、ケダル、アデベエル、ミブサム、ミシュマ、ドマ、マサ、ハダデ、テマ、エトル、ナフィシュ、ケデマ。

32アブラハムがそばめケトラに産ませた子は、ジムラン、ヨクシャン、メダン、ミデヤン、イシュバク、シュアハ。

ヨクシャンの子はシェバとデダン。

33ミデヤンの子はエファ、エフェル、エノク、アビダ、エルダア。

以上は、そばめケトラによるアブラハムの子孫です。

34アブラハムの子イサクには、エサウとイスラエルという二人の子がいました。

エサウの子孫

35エサウの子はエリファズ、レウエル、エウシュ、ヤラム、コラ。

36エリファズの子はテマン、オマル、ツェフィ、ガタム、ケナズ、ティムナ、アマレク。

37レウエルの子はナハテ、ゼラフ、シャマ、ミザ。

38-39セイルの子はロタン、ショバル、ツィブオン、アナ、ディション、エツェル、ディシャン、ロタンの妹ティムナ。

ロタンの子はホリとホマム。

40ショバルの子はアルヤン、マナハテ、エバル、シェフィ、オナム。

ツィブオンの子はアヤとアナ。

41アナの子はディション。

ディションの子はハムラン、エシュバン、イテラン、ケラン。

42エツェルの子はビルハン、ザアワン、ヤアカン。

ディシャンの子はウツとアラン。

43イスラエル王国が誕生する前に、エドムの地を治めていた王は次のとおりです。

ディヌハバの町に住んでいた、ベオルの子ベラ。

44ベラが死んで、ボツラ出身のゼラフの子ヨバブが新しく王となりました。

45ヨバブが死ぬと、テマン人の地出身のフシャムが王になりました。

46フシャムが死ぬと、モアブの野でミデヤン軍を打ち破ったベダデの子ハダデが王となり、アビテの町で治めました。

47ハダデが死んで、マスレカの町出身のサムラが王座につきました。

48サムラが死んで、ユーフラテス河畔の町レホボテ出身のサウルが新しく王となりました。

49サウルが死ぬと、アクボルの子バアル・ハナンが王になりました。

50バアル・ハナンが死んで、ハダデが王となり、パイの町で治めました。彼の妻はマテレデの娘で、メ・ザハブの孫娘に当たるメヘタブエルでした。

51-54ハダデが死んだ時のエドムの首長たちは、次のとおりです。ティムナ、アルワ、エテテ、オホリバマ、エラ、ピノン、ケナズ、テマン、ミブツァル、マグディエル、イラム。