第 96 篇
上帝是至高的君王
(平行經文:歷代志上16·23-33)
1你們要向耶和華唱新歌,
普世都要向耶和華歌唱。
2要向耶和華歌唱,稱頌祂的名,
天天傳揚祂的拯救之恩。
3要在列國述說祂的榮耀,
在萬民中述說祂的奇妙作為。
4因為耶和華無比偉大,
當受至高的頌揚;
祂超越一切神明,當受敬畏。
5列邦的神明都是假的,
唯獨耶和華創造了諸天。
6祂尊貴威嚴,
祂的聖所充滿能力和榮美。
7萬族萬民啊,
要把榮耀和能力歸給耶和華,
歸給耶和華!
8要把耶和華當得的榮耀歸給祂,
要帶著祭物到祂的院宇敬拜祂。
9你們當在聖潔的耶和華面前俯伏敬拜,
大地要在祂面前戰抖。
10要告訴列國:
「耶和華掌權,
祂使大地堅立不搖,
祂必公正地審判萬民。」
11願天歡喜,願地快樂,
願海和其中的一切都歡呼澎湃。
12願田野和其中的萬物都喜氣洋洋,
願林中的樹木都歡然讚美耶和華。
13因為祂要來審判大地,
祂要按公義審判世界,
憑祂的信實審判萬民。
Salimo 96
1Imbirani Yehova nyimbo yatsopano;
Imbirani Yehova dziko lonse lapansi.
2Imbirani Yehova, tamandani dzina lake;
lalikirani chipulumutso chake tsiku ndi tsiku.
3Lengezani ulemerero wake pakati pa mayiko,
ntchito zake zodabwitsa pakati pa mitundu yonse ya anthu.
4Pakuti wamkulu ndi Yehova ndipo ndi woyenera kwambiri kumutamanda;
ayenera kuopedwa kupambana milungu yonse.
5Pakuti milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi mafano,
koma Yehova analenga mayiko akumwamba.
6Ulemu ndi ufumu zili pamaso pake,
mphamvu ndi ulemerero zili mʼmalo ake opatulika.
7Perekani kwa Yehova, inu mabanja a anthu a mitundu ina,
perekani kwa Yehova ulemerero ndi mphamvu.
8Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake;
bweretsani chopereka ndipo mulowe mʼmabwalo ake.
9Lambirani Yehova mu ulemerero wa chiyero chake;
njenjemerani pamaso pake, dziko lonse lapansi.
10Nenani pakati pa mitundu ya anthu, “Yehova akulamulira.”
Dziko lonse lakhazikika molimba, silingasunthidwe;
Iye adzaweruza mitundu ya anthu molungama.
11Mayiko akumwamba asangalale, dziko lapansi likondwere;
nyanja ikokome, ndi zonse zili mʼmenemo;
12minda ikondwere pamodzi ndi chilichonse chili mʼmenemo.
Pamenepo mitengo yonse ya mʼnkhalango idzayimba ndi chimwemwe;
13idzayimba pamaso pa Yehova,
pakuti Iye akubwera kudzaweruza dziko lapansi;
adzaweruza dziko lonse mwachilungamo
ndi mitundu ya anthu onse mʼchoonadi.