詩篇 72 – CCBT & CCL

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

詩篇 72:1-20

第 72 篇

為君王祈禱

所羅門的詩。

1上帝啊,

求你將你的公正賜給王,

將你的公義賜給王的兒子。

2讓他憑公義審判你的子民,

按公平對待那些貧苦的人。

3願大山給百姓帶來繁榮,

小山帶來公義。

4願他保護百姓中受苦的人,

拯救貧窮的人,打倒欺壓者。

5只要日月尚存,

願百姓永遠敬畏你。

6願他的統治如春雨降在新割過的草場上,

又像甘霖滋潤大地。

7在他統治之下,

願義人興旺,國富民強,

如月長存。

8願他的疆域橫跨洋海,

幼發拉底河直到地極。

9願曠野的居民都來向他下拜,

敵人都仆倒在塵土中。

10他施示巴西巴的君王都來納貢稱臣。

11願君王都敬拜他,

萬國都事奉他。

12貧窮人呼求,他便搭救;

困苦人無助,他就伸出援手。

13他憐憫軟弱和貧困的人,

拯救貧困人的性命。

14他要救他們脫離別人的壓迫和暴力,

因為他愛惜他們的生命。

15願王壽命長久,

願人們將示巴的金子獻給他,

不斷為他禱告,

終日稱頌他。

16願遍地五穀豐登,

山頂上出產豐富,

黎巴嫩的密林。

願各城人口稠密如原野的青草。

17願他的名流芳百世,如日長存。

願萬國都因他而蒙福,

都稱頌他。

18以色列的上帝耶和華當受稱頌,

唯有祂行奇妙的事。

19願祂榮耀的名永受稱頌!

願普天下充滿祂的榮耀。

阿們!阿們!

20耶西的兒子大衛的禱告結束。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 72:1-20

Salimo 72

Salimo la Solomoni.

1Patsani mwana wa mfumu nzeru zanu zoweruzira mwa chilungamo,

Inu Mulungu mupatseni mwana wa mfumu chilungamo chanu.

2Iye adzaweruza anthu anu mwachilungamo,

anthu anu ozunzika mosakondera.

3Mapiri adzabweretsa chuma kwa anthu anu,

timapiri tidzabweretsa zipatso zachilungamo.

4Iye adzateteza ozunzika pakati pa anthu

ndi kupulumutsa ana a anthu osowa;

adzaphwanya ozunza anzawo.

5Adzakhala ndi moyo pa mibado yonse,

nthawi zonse pamene dzuwa ndi mwezi zikuwala.

6Iye adzakhala kugwa kwa mvula pa minda yolimidwa

ngati mivumbi yothirira dziko lapansi.

7Mʼmasiku a munthu wolungama adzakhazikika;

chuma chidzachuluka mpaka mwezi utaleka kuwala.

8Iye adzalamulira kuchokera ku nyanja ina mpaka ku nyanja ina

ndiponso kuchokera ku mtsinje mpaka ku malekezero a dziko lapansi.

9Mafuko a mʼchipululu adzawerama pamaso pake

ndipo adani ake adzanyambita fumbi.

10Mafumu a ku Tarisisi ndi a ku zilumba zakutali

adzabweretsa mitulo kwa iye,

mafumu a ku Seba ndi Seba

adzapereka mphatso kwa iyeyo.

11Mafumu onse adzamuweramira

ndipo mitundu yonse idzamutumikira.

12Pakuti iye adzawombola wosowa amene akulira,

wozunzika amene alibe wina womuthandiza.

13Iye adzachitira chifundo anthu ofowoka ndi anthu osowa

ndi kupulumutsa osowa ku imfa.

14Iye adzalanditsa iwo ku mazunzo ndi chiwawa

pakuti magazi awo ndi amtengo wapatali pamaso pake.

15Iye akhale ndi moyo wautali;

golide ochokera ku Seba apatsidwe kwa iye.

Anthu amupempherere nthawi zonse

ndi kumudalitsa tsiku lonse.

16Mulole kuti tirigu achuluke mʼdziko lonse;

pamwamba pa mapiri pakhale tirigu.

Zipatso zake zichuluke ngati za ku Lebanoni;

zichuluke ngati udzu wakuthengo

17Dzina lake likhazikike kwamuyaya,

lipitirire kukhala monga momwe limakhalira dzuwa.

Mitundu yonse idzadalitsika kudzera mwa iye

ndipo iwo adzamutcha iye wodala.

18Matamando akhale kwa Yehova Mulungu, Mulungu wa Israeli

amene Iye yekha amachita ntchito zodabwitsa.

19Matamando akhale ku dzina lake laulemerero kwamuyaya

dziko lonse lapansi lidzaze ndi ulemerero wake.

Ameni ndi Ameni.

20Uku ndiko kumaliza kwa mapemphero a Davide mwana wa Yese.