詩篇 54 – CCBT & CCL

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

詩篇 54:1-7

第 54 篇

祈求上帝的拯救

西弗人去告訴掃羅:「大衛藏在我們那裡」,那時大衛作了這首訓誨詩,交給樂長,用弦樂器。

1上帝啊,

求你憑你的名拯救我!

求你用你的大能為我伸冤!

2上帝啊,求你垂聽我的禱告,

留心我口中的話。

3因為傲慢的人起來攻擊我,

目無上帝的暴徒正尋索我的性命。(細拉)

4看啊,上帝幫助我,主扶持我,

5祂必使我的仇敵自作自受。

信實的上帝啊,

求你毀滅他們。

6耶和華啊,

我甘心樂意獻上祭物,

我要讚美你的名,

因為你的名是美善的。

7你拯救我脫離一切艱難,

讓我傲視仇敵。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 54:1-7

Salimo 54

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Ndakatulo ya Davide. Pamene anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ndipo anati, “Kodi Davide sakubisala pakati pathu.”

1Pulumutseni Inu Mulungu, mwa dzina lanu;

onetsani kuti ndine wosalakwa mwamphamvu yanu.

2Imvani pemphero langa, Inu Mulungu

mvetserani mawu a pakamwa panga.

3Alendo akundithira nkhondo;

anthu ankhanza akufunafuna moyo wanga,

anthu amene salabadira za Mulungu.

4Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa;

Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine.

5Lolani kuti choyipa chifike pa iwo amene amandichita chipongwe;

mwa kukhulupirika kwanu awonongeni.

6Ine ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu;

ndidzatamanda dzina lanu, Inu Yehova,

pakuti ndi labwino.

7Pakuti Iyeyo wandipulumutsa ku masautso anga onse,

ndipo maso anga apenya kupambana kwa pa adani anga.