詩篇 127 – CCBT & CCL

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

詩篇 127:1-5

第 127 篇

頌讚上帝的美善

所羅門上聖殿朝聖之詩。

1若不是耶和華建造房屋,

建造者的工作都是徒勞。

若不是耶和華保護城池,

守城者保持警覺也是徒然。

2你早起晚睡,

為生活操勞也是徒然,

唯有耶和華所愛的人才能安眠。

3兒女是耶和華所賜的禮物,

孩子是祂所給的賞賜。

4人年輕時生的兒女猶如戰士手中的箭。

5袋中裝滿了箭的人有福了!

他們在城門與仇敵爭論時,

必不致蒙羞。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 127:1-5

Salimo 127

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni.

1Yehova akapanda kumanga nyumba,

omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe.

Yehova akapanda kulondera mzinda,

mlonda akanangolondera pachabe.

2Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa

ndi kusagona msanga madzulo,

kuvutikira chakudya choti mudye,

pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.

3Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova,

ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.

4Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja

mwa munthu wankhondo.

5Wodala munthu

amene motengera mivi mwake mwadzaza.

Iwo sadzachititsidwa manyazi

pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.