詩篇 114 – CCBT & CCL

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

詩篇 114:1-8

第 114 篇

逾越節之歌

1以色列人離開埃及

雅各家從異國出來時,

2猶大成為上帝的聖所,

以色列成為祂的國度。

3大海看見他們就奔逃,

約旦河也倒流。

4大山如公羊一般跳躍,

小山像羊羔一樣蹦跳。

5大海啊,你為何奔逃?

約旦河啊,你為何倒流?

6大山啊,你為何如公羊一般跳躍?

小山啊,你為何像羊羔一樣蹦跳?

7大地啊,你要在主面前,

雅各的上帝面前戰抖,

8因為祂使磐石變成水池,

使岩石湧出泉水。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 114:1-8

Salimo 114

1Pamene Israeli anatuluka mu Igupto,

nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,

2Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu,

Israeli anasanduka ufumu wake.

3Nyanja inaona ndi kuthawa,

mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;

4mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna,

timapiri ngati ana ankhosa.

5Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa?

iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?

6inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna,

inu timapiri, ngati ana ankhosa?

7Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi,

pamaso pa Mulungu wa Yakobo,

8amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime,

thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.