創世記 5 – CCBT & CCL

Chinese Contemporary Bible (Traditional)

創世記 5:1-32

亞當的後代

1以下是關於亞當後代的記載。

上帝造人的時候,是照祂自己的形像造的。 2祂造了男人和女人,又賜福給他們,在創造他們的那日稱他們為「人」。 3亞當一百三十歲生了一子,長相酷似自己,給他取名叫塞特4亞當生了塞特以後,又活了八百年,生兒育女, 5九百三十歲去世。

6塞特一百零五歲生以挪士7之後又活了八百零七年,生兒育女, 8九百一十二歲去世。

9以挪士九十歲生該南10之後又活了八百一十五年,生兒育女, 11九百零五歲去世。

12該南七十歲生瑪勒列13之後又活了八百四十年,生兒育女, 14九百一十歲去世。

15瑪勒列六十五歲生雅列16之後又活了八百三十年,生兒育女, 17八百九十五歲去世。

18雅列一百六十二歲生以諾19之後又活了八百年,生兒育女, 20九百六十二歲去世。

21以諾六十五歲生瑪土撒拉22之後與上帝親密同行三百年,生兒育女, 23共活了三百六十五年。 24以諾與上帝親密同行,後來被上帝接去,不在世上了。

25瑪土撒拉一百八十七歲生拉麥26之後又活了七百八十二年,生兒育女, 27九百六十九歲去世。

28拉麥一百八十二歲生了一個兒子, 29取名叫挪亞5·29 希伯來文中「挪亞」與「安慰」諧音。,他說:「耶和華咒詛了大地,以致我們艱辛勞苦,這孩子必使我們從艱辛勞苦中得安慰。」 30拉麥挪亞之後,又活了五百九十五年,生兒育女, 31七百七十七歲去世。

32挪亞五百歲生雅弗

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Genesis 5:1-32

Mibado Kuyambira pa Adamu Mpaka Nowa

1Ndondomeko ya mibado ya Adamu ndi iyi:

Pamene Mulungu analenga munthu, anamulenga mʼchifaniziro cha Mulungu. 2Iye analenga mwamuna ndi mkazi. Anawadalitsa ndipo anawatcha “Munthu.”

3Pamene Adamu anali ndi zaka 130, anabereka mwana wamwamuna wofanana naye ndipo anamutcha Seti. 4Atabadwa Seti, Adamu anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. 5Zaka zonse za Adamu zinali 930 ndipo anamwalira.

6Pamene Seti anali ndi zaka 105, anabereka Enosi. 7Atabadwa Enosi, Seti anakhala ndi moyo zaka zina 807 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. 8Zaka zonse za Seti zinali 912 ndipo anamwalira.

9Pamene Enosi anali ndi zaka 90, anabereka Kenani. 10Atabadwa Kenani, Enosi anakhala ndi moyo zaka zina 815 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. 11Zaka zonse za Enosi pamodzi zinali 905 ndipo anamwalira.

12Pamene Kenani anali ndi zaka 70, anabereka Mahalaleli. 13Atabadwa Mahalaleli, Kenani anakhala ndi moyo zaka zina 840 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. 14Zaka zonse za Kenani zinali 910, ndipo anamwalira.

15Pamene Mahalaleli anali ndi zaka 65, anabereka Yaredi. 16Atabadwa Yaredi, Mahalaleli anakhala ndi moyo zaka zina 830 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. 17Zaka zonse za Mahalaleli zinali 895 ndipo anamwalira.

18Pamene Yaredi anali ndi zaka 162, anabereka Enoki. 19Atabadwa Enoki, Yaredi anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. 20Zaka zonse za Yaredi zinali 962 ndipo anamwalira.

21Pamene Enoki anali ndi zaka 65, anabereka Metusela. 22Atabadwa Metusela, Enoki anayenda ndi Mulungu zaka 300 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. 23Zaka zonse za Enoki zinali 365. 24Enoki anayenda ndi Mulungu; ndipo iye sanaonekenso chifukwa Mulungu anamutenga.

25Pamene Metusela anali ndi zaka 187, anabereka Lameki. 26Ndipo atabadwa Lameki, Metusela anakhala ndi moyo zaka zina 782 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. 27Zaka zonse za Metusela zinali 969, ndipo anamwalira.

28Pamene Lameki anali ndi zaka 182, anabereka mwana wamwamuna. 29Ndipo anamutcha Nowa ndipo anati, “Iyeyu adzatipumulitsa ku ntchito zathu zolemetsazi, zolima nthaka imene Yehova anayitemberera.” 30Atabadwa Nowa, Lameki anakhala zaka zina 595 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi. 31Zaka zonse za Lameki zinali 777, ndipo kenaka anamwalira.

32Pamene Nowa anali ndi zaka 500, anabereka Semu, Hamu ndi Yafeti.