诗篇 75 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

诗篇 75:1-10

第 75 篇

上帝是审判者

亚萨的诗,交给乐长,调用“休要毁坏”。

1上帝啊,

我们称谢你,我们称谢你,

因为你与我们同在。

人们都述说你奇妙的作为。

2你说:“我已定好时间,

我必秉公审判。

3大地震动,世人战抖的时候,

是我使地的根基稳固。(细拉)

4我警告狂妄人不要再狂傲,

告诫恶人不要再张狂。

5不要再狂妄自大,

不要说话傲气冲天。”

6人的尊贵不是来自东方,

不是来自西方,

也不是来自旷野。

7决定人尊贵的是上帝:

祂擢升这个,贬抑那个。

8耶和华手中的杯里盛满泛着泡沫、精工调制的怒酒。

祂倒出怒酒,让世上的恶人喝得一滴不剩。

9我要永远宣扬祂的作为,

我要颂赞雅各的上帝。

10上帝必铲除恶人的势力,

使义人充满力量。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 75:1-10

Salimo 75

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Salimo la Asafu. Nyimbo.

1Tikuthokoza Inu Mulungu,

tikuthokoza, pakuti dzina lanu lili pafupi nafe,

anthutu amafotokoza za ntchito zanu zodabwitsa.

2Mumati, “Ine ndimayika nthawi yoyenera,

ndine amene ndimaweruza mwachilungamo.

3Pamene dziko lapansi ndi anthu ake onse anjenjemera,

ndine amene ndimagwiriziza mizati yake molimba.

Sela

4Kwa odzitama ndikuti, ‘Musadzitamenso,’

ndipo kwa oyipa, ‘Musatukulenso nyanga zanu.

5Musatukule nyanga zanu motsutsana ndi kumwamba;

musayankhule ndi khosi losololoka.’ ”

6Kugamula milandu sikuchokera kummawa kapena kumadzulo

kapena ku chipululu.

7Koma ndi Mulungu amene amaweruza:

Iyeyo amatsitsa wina, nakwezanso wina.

8Mʼdzanja la Yehova muli chikho

chodzaza ndi vinyo wochita thovu, wosakanizidwa ndi zokometsera;

Iye amamutsanulira pansi ndipo onse oyipa a dziko lapansi

amamwa ndi senga zake zonse.

9Kunena za ine, ndidzalengeza izi kwamuyaya;

ndidzayimba matamando kwa Mulungu wa Yakobo.

10Ndidzadula nyanga za onse oyipa

koma nyanga za olungama zidzakwezedwa.