诗篇 136 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

诗篇 136:1-26

第 136 篇

上帝的慈爱永远长存

1你们要称谢耶和华,

因为祂是美善的,

祂的慈爱永远长存。

2你们要称谢万神之神,

因为祂的慈爱永远长存。

3你们要称谢万主之主,

因为祂的慈爱永远长存。

4要称谢那位独行奇事的,

因为祂的慈爱永远长存。

5要称谢那位用智慧创造诸天的,

因为祂的慈爱永远长存。

6要称谢那位在水上铺展大地的,

因为祂的慈爱永远长存。

7要称谢那位创造日月星辰的,

因为祂的慈爱永远长存。

8祂让太阳管理白昼,

因为祂的慈爱永远长存。

9祂让月亮星辰管理黑夜,

因为祂的慈爱永远长存。

10要称谢那位击杀埃及人长子的,

因为祂的慈爱永远长存。

11祂带领以色列人离开埃及

因为祂的慈爱永远长存。

12祂伸出臂膀施展大能,

因为祂的慈爱永远长存。

13要称谢那位分开海的,

因为祂的慈爱永远长存。

14祂引领以色列人走过海,

因为祂的慈爱永远长存。

15祂让法老和他的军兵葬身海,

因为祂的慈爱永远长存。

16要称谢那位带领其子民走过旷野的,

因为祂的慈爱永远长存。

17要称谢那位击杀强大君王的,

因为祂的慈爱永远长存。

18祂击杀了大能的君王,

因为祂的慈爱永远长存。

19祂击杀了亚摩利西宏

因为祂的慈爱永远长存。

20祂击杀了巴珊

因为祂的慈爱永远长存。

21祂把他们的土地赐给祂的子民作产业,

因为祂的慈爱永远长存。

22祂把他们的土地赐给祂的仆人以色列人作产业,

因为祂的慈爱永远长存。

23祂眷顾处于卑贱境地的我们,

因为祂的慈爱永远长存。

24祂拯救我们脱离仇敌,

因为祂的慈爱永远长存。

25祂赐食物给众生,

因为祂的慈爱永远长存。

26你们要称谢天上的上帝,

因为祂的慈爱永远长存。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 136:1-26

Salimo 136

1Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.

Pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

2Yamikani Mulungu wa milungu.

Pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

3Yamikani Ambuye wa ambuye,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

4Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

5Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

6Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

7Amene anapanga miyuni ikuluikulu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

8Dzuwa lilamulire usana,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

9Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

10Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

11Natulutsa Israeli pakati pawo,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

12Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

13Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

14Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

15Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

16Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

17Amene anakantha mafumu akuluakulu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

18Napha mafumu amphamvu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

19Siloni mfumu ya Aamori,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

20Ogi mfumu ya Basani,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

21Napereka dziko lawo ngati cholowa,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

22Cholowa cha mtumiki wake Israeli;

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

23Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

24Amene anatimasula kwa adani athu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

25Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

26Yamikani Mulungu wakumwamba,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.