约翰福音 16 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

约翰福音 16:1-33

圣灵的工作

1“我把这些事告诉你们,以免你们失去信心。 2人们将把你们赶出会堂,时候将到,杀害你们的人还以为是在事奉上帝。 3他们这样做,是因为他们根本不认识父,也不认识我。 4我把这些事提前告诉你们,是要叫你们到时候可以想起我曾跟你们讲过这些事。我以前没有告诉你们,那是因为我还跟你们在一起。

5“现在我要去差我来的父那里,你们没有人问我去哪里。 6因为我把这些事告诉了你们,你们心里充满了忧愁。 7然而,我把实情告诉你们,我去对你们是有益的,因为如果我不去,护慰者就不会来,我去了就会派祂到你们这里来。 8祂来了,就要在罪、义、审判方面责备世人。 9在罪方面责备他们,是因为他们不信我; 10在义方面责备他们,是因为我要去父那里,你们再也看不到我了; 11在审判方面责备他们,是因为这世界的王受了审判。

12“我还有许多事情要告诉你们,可是你们现在不能明白。 13等到真理之灵来了,祂会引导你们,让你们明白一切的真理。祂不凭自己说话,而是把祂所听见的和有关将来的事告诉你们。 14祂也要把从我那里领受的指示你们,使我得荣耀。 15因为父的一切都是我的,所以我才说祂要把从我那里领受的指示你们。

转忧为喜

16“不久,你们就见不到我了,再过不久,你们还会看见我。”

17几个门徒彼此议论说:“祂说,‘不久,你们就见不到我了,再过不久,你们还会看见我’,祂又说,‘因为我要去父那里’,这到底是什么意思呢? 18祂说‘不久’是什么意思呢?我们真不明白!”

19耶稣知道他们想问祂,就说:“你们在议论我刚才说的话是什么意思吗? 20我实实在在地告诉你们,你们将痛哭、哀号,世人却要欢喜;你们将忧愁,然而你们的忧愁将变为喜乐。 21妇人分娩时都会痛苦不已,但孩子生下来后,她就会因为这世界添了一个新生命而充满欢乐,忘掉了生产的痛苦。 22同样,现在你们有忧愁,但到我再见你们的时候,你们的心必欢喜,而且这份喜乐是谁也夺不去的。

23“到那一天,你们就什么也不用问我了。我实实在在地告诉你们,你们奉我的名无论向父求什么,祂都会赐给你们。 24你们从来没有奉我的名求过什么,你们现在求,就必得到,好使你们的喜乐满溢。

胜过世界

25“我一直用比喻跟你们讲这些事,不久,我就不再用比喻了,而是清楚地把父的事告诉你们。 26到那天,你们将要奉我的名祈求,我不是说我要为你们向父祈求。 27父爱你们,因为你们一直爱我,并且相信我来自上帝。 28我从父那里来到这个世界,现在我要离开这个世界回到父那里。”

29门徒说:“如今你直截了当地告诉我们,不再用比喻了。 30现在我们知道你无所不知,无需人向你发问,因此我们相信你来自上帝。”

31耶稣说:“你们现在相信吗? 32看啊!时候快到了,现在就是,你们将要分散,各自回家,只留下我一人。不过,我并非一人,因为父与我在一起。 33我把这些事告诉你们,是要叫你们在我里面有平安。你们在世上会有苦难,但你们要放心,我已经胜过这个世界。”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yohane 16:1-33

1“Ine ndakuwuzani zonsezi kuti musadzakhumudwe. 2Iwo adzakuchotsani mʼsunagoge mwawo. Kunena zoona, nthawi ikubwera imene aliyense amene adzakuphani adzaganiza kuti akutumikira Mulungu. 3Iwo adzachita zoterozo chifukwa sanadziwe Atate kapena Inenso. 4Ine ndakuwuzani izi kuti nthawi ikadzafika mudzakumbukire kuti Ine ndinakuchenjezani kale. Ine sindinakuwuzeni izi poyamba paja chifukwa ndinali nanu.”

Ntchito ya Mzimu Woyera

5“Tsopano Ine ndikupita kwa Iye amene anandituma koma palibe wina mwa inu akundifunsa kuti, ‘Kodi mukupita kuti?’ 6Muli ndi chisoni kwambiri chifukwa ndakuwuzani zimene. 7Komatu ndakuwuzani zoona. Ine ndikuti kuli bwino kwa inu kuti ndichoke. Ngati sindichoka, Nkhosweyo sidzabwera kwa inu, koma ngati Ine ndipita, ndidzamutumiza kwa inu. 8Iye akabwera, adzatsutsa dziko lapansi za uchimo, zachilungamo ndi zachiweruzo. 9Za uchimo, chifukwa anthu sakhulupirira Ine. 10Za chilungamo, chifukwa Ine ndi kupita kwa Atate, kumene simudzandionanso. 11Za chiweruzo, chifukwa wolamulira dziko lino lapansi waweruzidwa tsopano.

12“Ine ndili ndi zambiri zoti ndiyankhule nanu, koma simungathe kuzilandira tsopano. 13Koma pamene Iye, Mzimu wachoonadi, abwera, adzakutsogolerani mʼchoonadi chonse. Iye sadzayankhula mwa Iye yekha, adzayankhula zokhazo zimene wamva ndipo Iye adzakuwuzani zimene zikubwera. 14Iye adzalemekeza Ine chifukwa adzatenga za Ine nadzakudziwitsani. 15Zonse za Atate ndi zanga. Ichi nʼchifukwa chake Ine ndanena kuti Mzimu Woyera adzatenga kwa Ine zanga kuti muzidziwe.”

Chisoni cha Ophunzira Chisandulika Chimwemwe

16Yesu anapitiriza kuyankhula kuti, “Mwa kanthawi kochepa, simudzandionanso, ndipo patatha nthawi pangʼono mudzandionanso.”

17Ena a ophunzira ake anati kwa wina ndi mnzake, “Kodi Iye akutanthauza chiyani ponena kuti, ‘Mwa kanthawi kochepa, simudzandionanso,’ ndi ‘ndipo patatha nthawi pangʼono mudzandionanso,’ ndiponso ‘chifukwa ndikupita kwa Atate?’ ” 18Iwo anapitiriza kufunsana kuti, “Kodi akutanthauza chiyani, ‘kanthawi kochepa?’ Ife sitikumvetsetsa chimene Iye akuyankhula.”

19Yesu anadziwa kuti ankafuna kuti amufunse za zimenezi, choncho anawafunsa kuti, “Kodi mukufunsana wina ndi mnzake chimene Ine ndimatanthauza pamene ndinati, ‘Mwa kanthawi kochepa simudzandionanso,’ ndi ‘patatha nthawi pangʼono mudzandionanso?’ 20Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti inu mudzalira ndi kubuma pomwe dziko lapansi lidzakhale likukondwera. Inu mudzamva chisoni, koma chisoni chanu chidzasandulika chimwemwe. 21Mayi akamabereka mwana amamva ululu chifukwa nthawi yake yafika; koma mwana wake akabadwa amayiwala ululu wake chifukwa cha chimwemwe chake chakuti mwana wabadwa mʼdziko lapansi. 22Chimodzimodzinso ndi inu. Tsopano ino ndi nthawi yanu yomva chisoni, koma Ine ndidzakuonaninso ndipo inu mudzasangalala, ndipo palibe amene adzachotsa chimwemwe chanu. 23Tsiku limenelo inu simudzandipemphanso kalikonse. Ine ndikukuwuzani zoona kuti Atate anga adzakupatsani chilichonse chimene mudzapempha mʼdzina langa. 24Mpaka tsopano simunapemphe kalikonse mʼdzina langa. Pemphani ndipo mudzalandira, ndipo chimwemwe chanu chidzakhala chathunthu.

25“Ngakhale ndakhala ndikuyankhula mʼmafanizo, nthawi ikubwera imene Ine sindidzagwiritsanso ntchito mafanizo otere koma ndidzakuwuzani momveka za Atate anga. 26Tsiku limenelo inu mudzapempha mʼdzina langa. Ine sindikunena kuti ndidzapempha Atate mʼmalo mwanu ayi. 27Atate mwini anakukondani chifukwa inu mwandikonda Ine ndipo mwakhulupirira kuti Ine ndinabwera kuchokera kwa Atate. 28Ine ndinabwera kuchokera kwa Atate ndi kulowa mʼdziko lapansi. Tsopano ndikulisiya dziko lapansi kubwerera kwa Atate.”

29Kenaka ophunzira ake anati, “Tsopano mukuyankhula momveka bwino ndi mopanda mafanizo. 30Tsopano ife tikuona kuti Inu mumadziwa zinthu zonse ndi kuti sipafunika wina aliyense kukufunsani. Mwa ichi ife takhulupirira kuti Inu munachokera kwa Mulungu.”

31Yesu anawafunsa kuti, “Kodi tsopano mwakhulupirira?” 32Koma nthawi ikubwera ndipo yafika, pamene inu mudzabalalitsidwa, aliyense ku nyumba yake. Inu mudzandisiya ndekhandekha. Koma Ine sindili ndekha, pakuti Atate anga ali nane.

33“Ine ndakuwuzani izi kuti mwa Ine mukhale nawo mtendere. Mʼdziko lapansi mudzakhala nawo mavuto. Koma limbikani mtima! Ine ndaligonjetsa dziko lapansi.”