约伯记 26 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

约伯记 26:1-14

约伯的回答

1约伯回答说:

2“你真是帮了软弱者的大忙!

救了臂膀无力的人!

3无智慧的人真多亏你的指教!

承蒙你的真知灼见!

4谁帮你想出这些点子?

谁的灵在借着你发言?

5“阴魂和水族在水底战抖,

6阴间在祂面前裸露,

冥府毫无遮掩。

7祂将北极铺在空中,

将地悬在虚无中;

8祂将水卷在密云中,

云负重却不裂开。

9祂遮盖自己的宝座26:9 宝座”或译“满月”。

把云彩铺在上面。

10祂在海面上画出地平线,

作为光明与黑暗的交界。

11祂的斥责使天柱震动惊骇,

12祂的能力使大海平静,

祂运用智慧击碎海怪。

13祂吹散天上的阴霾,

挥手刺穿逃跑的蛇。

14看啊,这不过是祂作为的一斑,

是我们听到的少许回音!

谁能领悟祂的雷霆万钧?”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 26:1-14

Mawu a Yobu

1Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2“Wamuthandizadi munthu wopanda mphamvu!

Walimbitsadi dzanja la munthu wofowoka!

3Wapereka malangizo kwa munthu amene alibe nzeru!

Ndipotu waonetsadi nzeru zochuluka!

4Kodi wakuthandiza ndani kuti uyankhule mawu awa?

Ndipo ndi mzimu wa yani umene unayankhula pakamwa pako?

5“Mizimu ya anthu akufa ikunjenjemera pansi pa madzi,

ndi zonse zokhala mʼmadzimo.

6Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu;

chiwonongeko ndi chosaphimbidwa.

7Mulungu anayala thambo la kumpoto pa phompho;

Iye anakoloweka dziko lapansi mʼmalo mwake pamene panali popanda nʼkanthu komwe.

8Amasunga madzi ambiri mʼmitambo yake,

koma mitamboyo siphulika chifukwa cha kulemera kwa madziwo.

9Iye amaphimba mwezi wowala,

amawuphimba ndi mitambo yake.

10Mulungu anawalembera madzi malire wonga uta,

kukhala malire pakati pa kuwunika ndi mdima.

11Mizati yochirikiza mitambo yakumwamba imanjenjemera,

ndi kudabwa pa kudzudzula kwake.

12Ndi mphamvu zake anatontholetsa nyanja;

ndi nzeru zake anakantha chirombo cha mʼmadzi chija chotchedwa Rahabe.

13Ndi mpweya wake anayeretsa zamumlengalenga,

dzanja lake linapha chinjoka chothawa chija.

14Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake;

tingomva pangʼono za Iye ngati kunongʼona!

Kodi ndani angathe kudziwa kukula kwa mphamvu zake?”