提摩太后书 2 – CCB & CCL

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

提摩太后书 2:1-26

基督的精兵

1我儿啊!你要靠着基督耶稣的恩典刚强起来。 2以前你在许多见证人面前听过我的教导,你要把这些教导传给忠信可靠、能够教导他人的人。

3你要做基督耶稣的精兵与我同受苦难。 4当兵的若让其他事务缠身,就不能取悦征召他的上司。 5同样,参加比赛的人若不遵守比赛规则,就不可能得奖。 6辛劳的农夫理当先享受收成。 7你要思想我说的话,因为主必赐你悟性明白各样的事。

8你要切记我所传的福音:耶稣基督是大卫的后裔,祂从死里复活了。 9我为这福音受苦,甚至像犯人一样被囚禁,但上帝的道是囚禁不住的。 10我为了上帝所拣选的人忍受一切痛苦,使他们可以获得在基督耶稣里的救恩和永远的荣耀。 11有真实可信的话说:

“我们若与基督同死,

就必与祂同活。

12我们若忍耐到底,

就必与祂一同做王。

我们若不承认祂,

祂也必不承认我们。

13我们纵然会失信,

祂仍然信实可靠,

因为祂不能违背自己。”

做无愧的工人

14你要提醒众人这些事,在主面前嘱咐他们:不要为言词争辩,因为那对听见的人有害无益。 15你应当竭力在上帝面前做经得起考验、问心无愧的工人,正确地阐释真理之道。 16要远避一切世俗的空谈,因为好空谈的人只会越来越不敬虔。 17他们讲的话像毒疮,只会越烂越大,许米乃腓理徒就是例子。 18他们离经背道,说复活的事已成过去,动摇了许多人的信心。 19然而,上帝所立的坚实根基永不动摇,这根基上刻着:“主认识谁是属于祂的人”,“凡自称是属于主的人都要离弃罪恶。”

20大户人家不但有金器银器,也有木器瓦器,这些器皿的用途有贵贱之分。 21人若洁身自爱,远离卑贱的事,就必成为圣洁无瑕的贵重器皿,可以被主用来成就各样的善事。

22你要逃避年轻人的邪情私欲,要跟那些以清洁的心求告主的人一同追求公义、信心、仁爱、和平。 23不要参与愚昧无知的辩论,因为这些事只会引起纷争。 24上帝的奴仆不可与人争执,总要温和待人,善于教导,心存忍耐。 25要温柔地规劝那些反对我们的人,也许上帝会赐给他们悔改的心,使他们明白真理, 26让他们这些被魔鬼掳去、受其摆布的人能够醒悟过来,脱离魔鬼的网罗。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Timoteyo 2:1-26

1Tsono iwe, mwana wanga, limbika mʼchisomo chimene chili mwa Khristu Yesu. 2Ndipo zinthu zimene unamva ine ndikuziyankhula pamaso pa mboni zambiri, uziphunzitse kwa anthu odalirika amene akaphunzitsenso ena. 3Umve nane zowawa, monga msilikali wa Khristu Yesu. 4Palibe msilikali amene ali pa ntchito amagwiranso ntchito za anthu wamba, iye amafuna kukondweretsa bwana wolamulira. 5Chimodzimodzinso, munthu amene ali pa mpikisano waliwiro, salandira mphotho ya wopambana pokhapokha atatsiriza monga mwa malamulo a mpikisanowo. 6Mlimi wolimbika ndi amene amayembekezereka kukhala woyambirira kulandira gawo la zokolola. 7Lingalira zimene ndikunenazi, pakuti Ambuye adzakuzindikiritsa zonsezi.

8Kumbukira Yesu Khristu wochokera ku mtundu wa Davide kuti anauka kwa akufa. Uwu ndiye uthenga wanga wabwino 9umene ndikuwuvutikira choterewu mpaka kumangidwa ndi maunyolo ngati wakuba. Koma mawu a Mulungu sanamangidwe ndi maunyolo. 10Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha.

11Mawu oyenera kuwadalira ndi awa:

Ngati ife tinafa naye pamodzi,

tidzakhalanso moyo pamodzi naye.

12Ngati tinapirira,

tidzalamuliranso naye pamodzi.

Ngati ife timukana,

Iye adzatikananso.

13Ngati ndife osakhulupirika,

Iye adzakhalabe wokhulupirika

popeza sangathe kudzikana.

Kuthana ndi Aphunzitsi Onyenga

14Uziwakumbutsa anthu a Mulungu zinthu izi. Uwachenjeze pamaso pa Mulungu kuti asamakangane pa za mawu. Zimenezi nʼzopanda phindu ndipo zimangowononga amene akumvawo. 15Uyesetse kukhala wovomerezeka pamaso pa Mulungu monga wantchito wopanda chifukwa chochitira manyazi amene amalalikira mawu achoonadi molondola. 16Upewe nkhani zopanda pake, zosalemekeza Mulungu, chifukwa anthu oyankhula zotere amanka napotokerapotokera. 17Chiphunzitso chawo chidzafalikira ngati chilonda. Mwa anthuwa muli Humenayo ndi Fileto. 18Iwowa apatuka pa choonadi. Iwo amaphunzitsa kuti kuuka kwa akufa kunachitika kale, motero amawononga chikhulupiriro cha anthu ena. 19Komabe maziko olimba, amene Mulungu anawayika ngokhazikika, ndipo mawu olembedwapo ndi awa: “Yehova amadziwa amene ndi ake,” ndiponso, “Aliyense amene amavomereza dzina la Ambuye ayenera kusiya zoyipa.”

20Mʼnyumba yayikulu simukhala ziwiya zagolide ndi zasiliva zokha, koma mumakhalanso zamtengo ndi zadothi. Zina zimakhala za ntchito yapamwamba, zina za ntchito wamba. 21Munthu akadziyeretsa nʼkusiya ntchito za wambazi, adzakhala chiwiya cha ntchito yapamwamba, woyeretsedwa, ndi waphindu kwa Ambuye wake, wokonzeka kugwira ntchito iliyonse yabwino.

22Thawa zilakolako zoyipa zachinyamata. Funafuna chilungamo, chikhulupiriro, chikondi ndi mtendere pamodzi ndi amene akuyitanira pa dzina la Ambuye ndi mtima osadetsedwa. 23Ukane matsutsano oyipa ndi opusa, chifukwa amayambitsa mikangano. 24Ndiponso mtumiki wa Ambuye asamakangane ndi anthu, koma azikhala wachifundo kwa aliyense, wodziwa kuphunzitsa, osati wokalipakalipa. 25Otsutsana naye awalangize mofatsa, mwina Mulungu adzawapatsa mwayi woti asinthike ndi kuzindikira choonadi. 26Motero nzeru zawo zidzabweramo, ndipo adzathawa msampha wa mdierekezi, amene anawagwira ukapolo kuti azichita zofuna zake.