Песнь 140
Песнь Довуда.
1Вечный, я взываю к Тебе: поспеши ко мне!
Услышь моё моление, когда я взываю к Тебе.
2Прими молитву мою,
как возжигание благовоний перед Тобой,
и возношение моих рук –
как вечернее жертвоприношение.
3Поставь, Вечный, стражу у моего рта,
стереги двери моих уст.
4Не дай моему сердцу склониться к злу,
не дай участвовать в беззаконии нечестивых,
и не дай вкусить от их сластей.
5Пусть накажет меня праведник – это милость;
пусть обличает меня – это лучшее помазание,
которое не отринет моя голова.
Но моя молитва против злодеев:
6да будут вожди их сброшены с утёсов.
Тогда люди узнают,
что мои слова были правдивы.
7Как земля, которую рассекают и дробят,
так рассыпаны наши кости у пасти мира мёртвых.
8Но глаза мои устремлены на Тебя, Владыка Вечный;
на Тебя надеюсь, не дай мне умереть!
9Сохрани меня от сетей, которые раскинули для меня,
и от западни злодеев.
10Пусть нечестивые падут в свои же сети,
а я их избегу.
Salimo 140
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
1Landitseni Yehova kwa anthu oyipa;
tetezeni kwa anthu ankhanza,
2amene mu mtima mwawo amakonza zinthu zoyipa
ndi kuyambitsa nkhondo tsiku lililonse.
3Iwo amanola malilime awo kukhala akuthwa ngati a njoka;
pa milomo yawo pali ululu wa mamba.
Sela
4Tetezeni Inu Yehova, kwa anthu oyipa;
tchinjirizeni kwa anthu ankhanza
amene amakonza zokola mapazi anga.
5Anthu odzikuza anditchera msampha mobisika;
iwo atchera zingwe za maukonde awo
ndipo anditchera misampha pa njira yanga.
Sela
6Inu Yehova, ine ndikuti, “Ndinu Mulungu wanga.”
Imvani kupempha kwanga Yehova.
7Inu Ambuye Wamphamvuzonse, Mpulumutsi wanga wamphamvu,
mumateteza mutu wanga tsiku lankhondo.
8Musawapatse anthu oyipa zokhumba zawo, Inu Yehova;
musalole kuti zokonza zawo zitheke,
mwina iwo adzayamba kunyada.
Sela
9Mitu ya amene andizungulira
iphimbidwe ndi masautso amene milomo yawo yayambitsa.
10Makala amoto agwere pa iwo;
aponyedwe pa moto,
mʼmaenje amatope, asatulukemonso.
11Musalole kuti anthu achipongwe akhazikike mʼdziko;
choyipa chilondole anthu ankhanza.
12Ndikudziwa kuti Yehova amapereka chiweruzo cholungama kwa anthu osauka,
ndipo amateteza zolinga za anthu osowa.
13Zoonadi anthu olungama adzatamanda dzina lanu,
ndipo anthu owongoka mtima adzakhala pamaso panu.