Забур 133 – CARST & CCL

Священное Писание (Восточный перевод), версия для Таджикистана

Забур 133:1-3

Песнь 133

Песнь восхождения.

1Славьте Вечного, все рабы Его,

служащие ночью в доме Вечного!

2Вознесите руки свои в святилище

и славьте Вечного!

3Вечный, сотворивший небо и землю,

да благословит тебя с Сиона.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 133:1-3

Salimo 133

Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu

pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!

2Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu,

otsikira ku ndevu,

ku ndevu za Aaroni,

oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.

3Zili ngati mame a ku Heremoni

otsikira pa Phiri la Ziyoni.

Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso,

ndiwo moyo wamuyaya.