Забур 125 – CARST & CCL

Священное Писание (Восточный перевод), версия для Таджикистана

Забур 125:1-6

Песнь 125

Песнь восхождения.

1Когда Вечный вернул благополучие Сиону,

мы были как бы во сне.

2Тогда мы смеялись

и пели радостные песни.

Тогда говорили народы:

«Великие дела сотворил для них Вечный».

3Великие дела сотворил для нас Вечный,

и мы полны радости.

4Верни нам благополучие, Вечный,

как высохшие русла рек в пустыне Негев

вновь наполняются водой.

5Сеявшие со слезами

будут пожинать с радостью.

6С плачем несущий суму с семенами

с радостью возвратится,

неся свои снопы.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 125:1-5

Salimo 125

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,

limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.

2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,

momwemonso Yehova azungulira anthu ake

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala

pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama,

kuti anthu olungamawo

angachite nawonso zoyipa.

4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,

amene ndi olungama mtima

5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,

Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa.

Mtendere ukhale pa Israeli.