Песнь 137
Песнь Давуда.
1Буду славить Тебя всем своим сердцем;
перед богами137:1 Боги – слово, стоящее здесь на языке оригинала, имеет более широкое значение и в данном случае обозначает либо ангелов, либо земных правителей, судей или священнослужителей, либо языческих богов. воспою хвалу Тебе.
2Поклонюсь пред святым храмом Твоим
и буду славить имя Твоё
за Твою милость и верность,
потому что Ты обещал мне больше,
чем я мог ожидать137:2 Букв.: «Ты превознёс Твоё слово превыше всякого Твоего имени»..
3В день, когда я воззвал, Ты ответил мне,
ободрил и укрепил мою душу.
4Вечный, все земные цари будут славить Тебя,
когда услышат слова из уст Твоих.
5Они воспоют пути Вечного,
потому что велика слава Вечного.
6Высок Вечный, но заботится о смиренном
и высокомерного узнаёт издали.
7Даже если пойду я среди несчастья,
Ты оживишь меня,
защитишь от ярости моих врагов,
и спасёт меня Твоя правая рука.
8Вечный свершит то, что задумал для меня.
Твоя милость, Вечный, навеки:
не оставляй творения Твоих рук!
Salimo 137
1Mʼmbali mwa mitsinje ya ku Babuloni tinakhala pansi ndi kulira
pamene tinakumbukira Ziyoni.
2Kumeneko, pa mitengo ya misondozi
tinapachika apangwe athu,
3pakuti anthu otigwira ukapolo anatipempha kuti tiyimbe nyimbo.
Otizunza athu anafuna nyimbo zachisangalalo;
iwo anati, “Tiyimbireni imodzi mwa nyimbo za ku Ziyoni!”
4Tingayimbe bwanji nyimbo za Yehova
mʼdziko lachilendo?
5Ndikakuyiwala iwe Yerusalemu,
dzanja langa lamanja liyiwale luso lake.
6Lilime langa limamatire ku nkhama za mʼkamwa mwanga
ndikapanda kukukumbukira iwe Yerusalemu,
ngati sindiyesa iwe
chimwemwe changa chachikulu.
7Kumbukirani, Inu Yehova, zimene Aedomu anachita
pa tsiku limene Yerusalemu anagonja.
Iwowo anafuwula kuti, “Mugwetseni pansi, mugwetseni pansi
mpaka pa maziko ake!”
8Iwe mwana wa mkazi wa Babuloni, woyenera kuwonongedwa,
wodalitsika ndi yemwe adzakubwezera
pa zimene watichitira.
9Amene adzagwira makanda ako
ndi kuwakankhanthitsa pa miyala.