Песнь 121
Песнь восхождения, Давуда.
1Обрадовался я, когда мне сказали:
«Пойдём в храм Вечного».
2Ноги наши стоят
у ворот твоих, Иерусалим.
3Иерусалим – плотно застроенный город.
4Туда поднимаются роды,
роды Вечного,
по Закону Исраила,
воздать хвалу имени Вечного.
5Там стоят престолы суда,
престолы дома Давуда.
6Молитесь о мире для Иерусалима:
«Пусть будут благополучны любящие тебя.
7Пусть будет мир в твоих стенах
и благополучие в твоих дворцах».
8Ради моей семьи и моих друзей
скажу: «Мир тебе!»
9Ради храма Вечного, нашего Бога,
желаю блага тебе.
Salimo 121
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1Ndikweza maso anga ku mapiri;
kodi thandizo langa limachokera kuti?
2Thandizo langa limachokera kwa Yehova,
wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3Sadzalola kuti phazi lako literereke;
Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4Taonani, Iye amene amasunga Israeli
sadzawodzera kapena kugona.
5Yehova ndiye amene amakusunga;
Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,
kapena mwezi nthawi ya usiku.
7Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;
adzasunga moyo wako.
8Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;
kuyambira tsopano mpaka muyaya.