Забур 121 – CARS & CCL

Священное Писание

Забур 121:1-9

Песнь 121

Песнь восхождения, Давуда.

1Обрадовался я, когда мне сказали:

«Пойдём в храм Вечного».

2Ноги наши стоят

у ворот твоих, Иерусалим.

3Иерусалим – плотно застроенный город.

4Туда поднимаются роды,

роды Вечного,

по Закону Исраила,

воздать хвалу имени Вечного.

5Там стоят престолы суда,

престолы дома Давуда.

6Молитесь о мире для Иерусалима:

«Пусть будут благополучны любящие тебя.

7Пусть будет мир в твоих стенах

и благополучие в твоих дворцах».

8Ради моей семьи и моих друзей

скажу: «Мир тебе!»

9Ради храма Вечного, нашего Бога,

желаю блага тебе.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 121:1-8

Salimo 121

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Ndikweza maso anga ku mapiri;

kodi thandizo langa limachokera kuti?

2Thandizo langa limachokera kwa Yehova,

wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.

3Sadzalola kuti phazi lako literereke;

Iye amene amakusunga sadzawodzera.

4Taonani, Iye amene amasunga Israeli

sadzawodzera kapena kugona.

5Yehova ndiye amene amakusunga;

Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.

6Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,

kapena mwezi nthawi ya usiku.

7Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;

adzasunga moyo wako.

8Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;

kuyambira tsopano mpaka muyaya.