Salmernes Bog 67 – BPH & CCL

Bibelen på hverdagsdansk

Salmernes Bog 67:1-8

Under Guds velsignelse

1Til korlederen: Brug strengeinstrumenterne. En lovsang.

2Velsign os og vær os nådig, Gud.

Grib ind og udfør dine undere.

3Alle jordens folk vil kunne se, hvem du er,

når de oplever din magt til at frelse.

4Alle folkeslag på jorden skal prise dig, Gud,

alle verdens nationer skal give dig ære.

5Alle folkeslagene skal fryde sig over dig,

de vil lovprise dig med glædessange,

for alle dine handlinger er retfærdige,

og du regerer over alle nationer.

6Alle folkeslag på jorden skal prise dig, Gud,

alle verdens nationer skal give dig ære.

7Du har velsignet os, Gud,

og givet os en god høst.

8Når Gud velsigner os mennesker så rigt,

bør alle folkeslag på jorden give ham ære.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 67:1-7

Salimo 67

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo.

1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

achititse kuti nkhope yake itiwalire.

2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.

3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo

ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.

5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

6Nthaka yabereka zokolola zake;

tidalitseni Mulungu wathu.

7Mulungu atidalitse

kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.