Psaumes 131 – BDS & CCL

La Bible du Semeur

Psaumes 131:1-3

Calme souverain

1Cantique pour la route vers la demeure de l’Eternel131.1 Voir note 120.1.. De David.

O Eternel, ╵mon cœur ne s’enfle pas d’orgueil, ╵mes yeux n’ont pas visé trop haut,

je ne me suis pas engagé ╵dans des projets trop grands,

trop compliqués pour moi.

2Bien au contraire : ╵je suis resté tranquille et calme,

comme un enfant sevré ╵porté par sa maman.

Oui, je me sens au fond de moi ╵comme l’enfant sevré.

3Israël, mets ta confiance ╵en l’Eternel,

dès maintenant et pour toujours.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 131:1-3

Salimo 131

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide.

1Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza,

maso anga siwonyada;

sinditengeteka mtima

ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.

2Koma moyo wanga ndawutontholetsa

ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa,

moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.

3Yembekeza Yehova, iwe Israeli,

kuyambira tsopano mpaka muyaya.