Nnwom 98 – AKCB & CCL

Akuapem Twi Contemporary Bible

Nnwom 98:1-9

Dwom 98

Dwom.

1Monto dwom foforo mma Awurade,

efisɛ wayɛ anwonwade bebree;

ne nsa nifa ne ne basa kronkron no

anya nkwagye ama no.

2Awurade ama wɔahu ne nkwagye

na wada ne trenee adi akyerɛ amanaman no.

3Wakae nʼadɔe

ne ne nokware a odi kyerɛɛ Israelfo no;

asase ano nyinaa ahu

yɛn Nyankopɔn nkwagye.

4Asase nyinaa mommɔ ose mma Awurade,

momfa nnwonto nni ahurusi;

5Momfa sanku nto dwom mma Awurade,

sanku ne nnwonto nnyigyei,

6momfa torobɛnto ne adwennini mmɛn,

nteɛ mu ahosɛpɛw so wɔ Awurade, yɛn hene no anim.

7Momma po ne abɔde a ɛwɔ mu nyinaa nhuru so;

asase ne wɔn a wɔte so nyinaa.

8Momma nsubɔnten mmɔ wɔn nsam,

mmepɔw nka mmom nto ahurusi nnwom;

9ma wɔnto nnwom wɔ Awurade anim,

efisɛ ɔreba abebu wiase atɛn.

Ɔde trenee bebu wiase atɛn

na ɔde pɛpɛyɛ abu nnipa atɛn.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 98:1-9

Salimo 98

Salimo.

1Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,

pakuti Iyeyo wachita zinthu zodabwitsa;

dzanja lake lamanja ndi mkono wake woyera

zamuchitira chipulumutso.

2Yehova waonetsa chipulumutso chake

ndipo waulula chilungamo chake kwa anthu a mitundu ina.

3Iye wakumbukira chikondi chake

ndi kukhulupirika kwake pa Aisraeli;

malekezero onse a dziko lapansi aona

chipulumutso cha Mulungu wathu.

4Fuwulani mwachimwemwe kwa Yehova, dziko lonse lapansi,

muyimbireni nyimbo mofuwula ndi mokondwera.

5Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze,

ndi zeze ndi mawu a kuyimba,

6ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna

fuwulani mwachimwemwe pamaso pa Yehova Mfumu.

7Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo,

dziko lonse ndi onse amene amakhala mʼmenemo.

8Mitsinje iwombe mʼmanja mwawo,

mapiri ayimbe pamodzi mwachimwemwe;

9izo ziyimbe pamaso pa Yehova,

pakuti Iye akubwera kudzaweruza dziko lapansi.

Adzaweruza dziko lonse mwachilungamo,

ndi mitundu ya anthu mosakondera.