Nnwom 57 – AKCB & CCL

Akuapem Twi Contemporary Bible

Nnwom 57:1-11

Dwom 57

Dawid dwom a ɔtoo bere a oguan fii Saulo nkyɛn kɔɔ ɔbodan no mu.

1Hu me mmɔbɔ, me Onyankopɔn, hu me mmɔbɔ,

na wo mu na me kra nya guankɔbea.

Wo ntaban nwini ase na mɛpɛ guankɔbea

kosi sɛ amanehunu no betwa mu.

2Misu frɛ Onyankopɔn, Ɔsorosoroni no;

Onyankopɔn a ɔma ne pɛ ba mu wɔ me ho.

3Ɔsoma fi ɔsoro hɔ begye me nkwa,

ɔka wɔn a wɔtaa me anibere so no anim;

Onyankopɔn soma ne dɔ ne ne nokware.

4Gyata atwa me ho ahyia;

meda mmoa a wɔwe nam amono mu,

nnipa a wɔn se te sɛ mpeaw ne mmɛmma

na wɔn tɛkrɛma te sɛ afoa a ɛyɛ nnam.

5Onyankopɔn, ɛsɛ sɛ wɔma wo so tra ɔsoro,

na ama wʼanuonyam aba asase nyinaa so.

6Wɔtrɛw asau mu de sum mʼanan afiri,

ahohiahia brɛɛ me ase.

Wotuu amoa wɔ me kwan mu,

nanso wɔn ankasa akɔtotɔ mu.

7Ao, Onyankopɔn, me koma agyina pintinn,

me koma yɛ pintinn;

mɛto dwom na mayi wo ayɛ.

8Me kra nyan!

Sanku ne bɛnta, munnyan!

Me nso menyan anɔpahema.

9Awurade, mɛkamfo wo wɔ aman no mu;

mɛto wo ho nnwom wɔ nnipa mu.

10Wʼadɔe so, ɛkorɔn sen ɔsoro;

wo nokwaredi du wim.

11Ao, Onyankopɔn, wɔmma wo so mmoro ɔsoro;

ma wʼanuonyam nkata asase nyinaa so.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 57:1-11

Salimo 57

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Ndakatulo ya Davide, pamene anathawa Sauli kupita ku phanga.

1Mundichitire chifundo, Inu Mulungu mundichitire chifundo,

pakuti mwa Inu moyo wanga umathawiramo.

Ndidzathawira mu mthunzi wa mapiko anu

mpaka chiwonongeko chitapita.

2Ine ndikufuwulira kwa Mulungu Wammwambamwamba,

kwa Mulungu amene amakwaniritsa cholinga chake pa ine.

3Mulungu amanditumizira kuchokera kumwamba ndi kundipulumutsa,

kudzudzula iwo amene akundithamangitsa kwambiri.

Mulungu amatumiza chikondi chake ndi kukhulupirika kwake.

4Ine ndili pakati pa mikango,

ndagona pakati pa zirombo zolusa;

anthu amene mano awo ndi milomo yawo ndi mivi,

malilime awo ndi malupanga akuthwa.

5Mukwezekedwe Inu Mulungu, kuposa mayiko onse akumwamba;

mulole kuti ulemerero wanu ukhale pa dziko lonse lapansi.

6Iwo anatchera mapazi anga ukonde

ndipo ndinawerama pansi mosautsidwa.

Anakumba dzenje mʼnjira yanga

koma agweramo okha mʼmenemo.

7Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu

mtima wanga ndi wokhazikika.

Ndidzayimba nyimbo, nyimbo yake yamatamando.

8Dzuka moyo wanga!

Dzukani zeze ndi pangwe!

Ndidzadzuka mʼbandakucha.

9Ndidzakutamandani Ambuye, pakati pa mitundu ya anthu,

ndidzayimba za Inu pakati pa mayiko.

10Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kufikira ku mayiko akumwamba;

kukhulupirika kwanu kwafika ku mitambo.

11Mukwezekedwe Inu Mulungu kuposa mayiko akumwamba,

mulole kuti ulemerero wanu ukhale pa dziko lonse lapansi.